ANATCHEZERA

ANATCHEZERA

Anatchezera

Takulandiraninso mu 2021 Ndikufuna ndikulandireni m’chaka cha 2021. Chaka chatha lidali thumba la zambiri. M’chakachi zina zidali zokoma, koma zina...

Anatchezera

Akukana banja Gogo, Ndidapalana ubwenzi ndi mtsikana wina chaka chatha. Ndimtsikana wokongola, komanso waulemu. Chomwe chimandidabwita n’choti ndikamuuza zabanja amakana....

Anatchezera

Akufuna mwana Gogo, Ndakhala m’banja ndi mwamuna wanga zaka zisanu, koma wopanda mwana. Mwamuna wanga amalimbitsa mtima kuti ndisadandaule popeza...

Anatchereza

Agogo ndili ndi zibwenzi ziwiri koma onsewo ndi pachibale komanso amadziwana. Ndikawauza kuti andisiye onse amakana, nditani gogo chifukwa onse...

Anatchereza

Akufuna mwana Gogo, Ndakhala m’banja ndi mwamuna wanga zaka zisanu, koma wopanda mwana. Mwamuna wanga amalimbitsa mtima kuti ndisadandaule popeza...

Anatchereza

Ndipite kwa asing’anga? Zikomo Anatchereza, Palitu mkazi amene amandizunguza bongo. Mtima wanga nthawi zonse umakhala pa iye ndipo sindigona tulo...

Anatchezera

Akufuna mwana Gogo, Ndakhala m’banja ndi mwamuna wanga zaka zisanu, koma wopanda mwana. Mwamuna wanga amalimbitsa mtima kuti ndisadandaule popeza...

ANatchereza

Sakufuna kukaonekera Gogo Natchereza, Mnyamata wina adandifunsira chibwenzi ndi cholinga choti tidzakwatirane. Padakali pano padutsa zaka zinayi tili paubwenzi, koma...

Anatchezera

Sakufuna kukaonekera Gogo Natchereza, Mnyamata wina adandifunsira chibwenzi ndi cholinga choti tidzakwatirane. Padakali pano padutsa zaka zinayi tili paubwenzi, koma...

anatchezera

Akundidabwitsa Anatchereza, Ndili pa chibwenzi ndi mwamuna wina. Chomwe chimandidabwitsa n’choti nthawi zonse ndikamuimbira foni usiku samayankha. Ndikamufunsa amati idali...

Anatchereza

Ndikufuna kuchoka Zikomo Anatchereza, Ndidabwera kutauni kudzafuna ntchito ndipo ndidasiya mkazi wanga kumudzi. Ntchito ndidaipeza koma abale amene ndimakhala m’nyumba...

Anatchezera

Ukuchita njomba Gogo Natcheteza, Ndine mtsikana wa zaka 25 ndipo ndakhala pa chibwenzi ndi mnyamata wina kwa zaka zinayi. Mnyamatayu...

Anatchezera

Akundifunanso Anatchereza, Telemu yotsiriza ya Fomu 3 ndidapalana ubwenzi ndi mtsikana wina pasukulu yathu ku Mulanje. Koma tikuyandikira kulemba mayeso...

ANATCHEZERA

Adandichotsa ntchito Zikomo Gogo Ndakhala ndikugwira ntchito kwa bwana wina mumzinda wa Blantyre kwa zaka 4. Masiku apitawa ndidaapempha holide...

Anatchereza

Mkazi wanga koma mkonono Agogo, Langa ndi dandaulo pa mkazi wanga wokondeka. Iyetu mwano alibe ndiponso ntchito amagwira molimbika. Abale...

Anatchezera

Akunyengana ndi mnzanga Zikomo Anatchereza, Ndakhala pabanja zaka 7 ndipo tilinso ndi mwana wa zaka 7. Tsiku lina mwanayo adathyoka...

Anatchezera

ANATCHEREZA Akundikakamira Ndili ndi mkazi yemwe ndili naye mwana mmodzi. Vuto lake ndi limodzi: amakhalira kunyoza makolo ndi abale anga....

Page 1 of 4 1 2 4

Opinions and Columns