-
National News
Road Traffic named most secretive
Media Institute of Southern Africa (Misa) Malawi Chapter has asked authorities at the Directorate of Road Traffic and Safety…
Read More » -
Chichewa
‘Aoloka yorodani’ pamtsinje wa ruo
Sukulu adalekera sitandade 4, kuwerenga n’komuvuta, koma kuwerengera ndalama kwa iye si nkhani. Ngakhale sukulu sadapite nayo patali, ntchito…
Read More » -
Asimba za kasamalidwe ka mpunga
M’maboma a Nsanje, Chikwawa, Machinga komanso maboma ena kuchigawo cha kumpoto alimi a mpunga ali kalikiriki ndi ulimi wa mpunga…
Read More » -
Nkhani
Alimi avale dzilimbe, kukubwera El Nino
Akatswiri a zanyengo alosera kuti chaka chino pali mantha kuti dziko lino lingakumane ndi nyengo yoipa ya El Nino. Lipoti…
Read More » -
Nkhani
Boma litemera ziweto 10 000
Pofuna kuthana ndi mliri wa matenda a zilonda za m’ mapazi ndi m’mkamwa a ng’ombe omwe agwa m’boma la Chikwawa,…
Read More » -
Nkhani
Malawi sisewera ndi Uganda
Chiyembekezo chidalipo kuti Malawi iswana ndi Uganda kuti ikonzekere masewero a World Cup pa 7 October pamene ikunthane ndi Tanzania.…
Read More » -
Nkhani
Mwambo ‘wopha mudzi’ poika mfumu
Anthu ena amakhulupirira kuti akamwalira amayenera akaikidwe chatsonga kapena kuti chokhala. Izi zimachitika kwambiri pakati pa mafumu Achingoni maka a…
Read More » -
Nkhani
Adutse ndani mu Standard Bank?
Ndime ya kotafainolo mu Standard Bank Cup yafika podetsa nkhawa pamene matimu anayi akuyenera kutsanzikana ndi chikhochi sabata ino. Pamene…
Read More » -
Nkhani
Anjata wopezeka ndi mitengo ya tsanya
Apolisi ku Lilongwe Lachitatu adanjata nzika ya ku China chifukwa chomuganizira kuti adapezeka ndi mitengo ya tsanya yomwe nzikayo imafuna…
Read More » -
Chichewa
‘Chidwi pantchito ya uphunzitsi chizilala’
Bungwe la aphunzitsi m’dziko muno la Teachers Union of Malawi (TUM) lati zomwe lachita boma pokhazikitsa mfundo yoti ofuna kuphunzira…
Read More » -
Ruo asokoneza za uchembere wabwino
Adali madzulo a pa 12 March 2015 pamene matenda a mayi Madalitso Ofeni, wa zaka 35, adakula. Nthawi ili…
Read More » -
Nkhani
Azula chamba, achiyatsa ku KK
Nkhani zoti apolisi alanda kapena azula chamba ndi zina zokhudza mbewu yozunguzayi sizikukata m’boma la Nkhotakota. Lachiwiri sabata ino apolisi…
Read More » -
Nkhani
Bullets yayamba ndi ukali
Timu ya Big Bullets, yomwe ikuteteza chikho cha TNM Super League, yayambanso ndi ukali m’ndime yachiwiri ya ligiyi, kupitiriza zomwe…
Read More » -
Nkhani
FAM ndi Kamuzu Stadium
Sabata yatha kwathu kuno kudabwera alendo a Fifa kudzayendera bwalo la Kamuzu Stadium ngati ndi loyenera kuti mipikisano ya chikho…
Read More » -
Nkhani
Mwambo woika maliro a khanda lozizira
Amalawi ngakhale ali ndi miyambo yosiyanasiyana malinga ndi mitundu yawo monga Achewa, Angoni, Atumbuka, Alhomwe, Amang’anga, Asena kaya ndi Ayao,…
Read More » -
Nkhani
Panazale samakololapo!
Flames yalepherana mphamvu ndi Swaziland 2-2 kusonyeza kuti m’gulu L la mpikisano wolimbirana chiko cha Africa Cup of Nations (Afcon)…
Read More » -
A maufulu ayamikira MCP
Akatswiri andale kudzanso mabungwe oimira ufulu wa anthu mdziko muno ayamikila chipani chachikulu chotsutsa boma cha Malawi Congress Party (MCP)…
Read More » -
Nkhani
‘Zilango zophweka zivulaza maalubino’
Miyezi 18 kwa ofuna kugulitsa alubino ku DZ Pali mantha kuti maalubino angapitirire kuona zokhoma m’dziko muno ngati boma silichita…
Read More » -
Dz Young Soccer, ‘Mighty’ adutsa
Chikho cha Standard Bank chayamba ndi moto pamene matimu a asirikali a Kamuzu Barracks ndi Mafco FC aona msana wa…
Read More » -
Nkhani
Mwambo woliza mfuti pamaliro Achingoni
Mfumu Yachingoni ikagona, pamaliropo amaomba mfuti thupi la mfumuyo lilowe m’manda. Mwezi wathawu, kudachitika maliro a T/A Bvumbwe m’boma la…
Read More »