-
Chichewa
‘JB asabisalire kwa amphawi za kuyenda’
Mtsogoleri wa dziko lino Joyce Banda wamenyetsa nkhwangwa pamwala ponena kuti, zivute zitani, sangasiye kuyendera anthu m’midzimu ndipo wati zikafika…
Read More » -
Ntchito yomanga njanji ya ku Nkaya yaima
Ntchito yomanga njanji yochoka ku Kachaso kupita ku Nkaya ayiimitsa mpaka kampani ya Mota-Engel ndi ogwira ntchito kukampaniyo atamvana chimodzi.…
Read More » -
Nkhani
Mgwirizano wabooka?
Amati “apolisi tisamawanyoze ndi abale athu”, koma zayambika m’dziko muno ndi chipolowe pamene anthu akuthotha apolisi ndi kusasula ofesi zawo…
Read More » -
Kodi za Gaba zalowa?
M’sabatayi aganyu tidali osangalala kumva kuti chilombo cha ukonde, Gabadihno Mhango, mwana wa Flames, tsopano wayamba kusewerera m’timu yatsopano ya…
Read More » -
Nkhani
Kampani yatsopano ikatamutsa alimi
Kampani yatsopano yogula ndi kugulitsa zakumunda ya Auction Holdings Limited Commodities Exchange (AHCX) yamema alimi kuti akagulitse mbewu zawo kubungweli…
Read More » -
National News
PostNL, WFP happy with school projects in Nsanje
The World Food Programme (WFP) and PostNL have expressed satisfaction with progress of primary school and early childhood development programmes…
Read More » -
National Sports
Big Bullets yaboola jombo, ipha KB 2-1
Sadyeka akupitirila kudyeka m’mafupa omwe, inde jombo yomwe yakhala ikumvetsa mutu matimu omwe si achisilikali tsopano akubooka. Lero timu ya…
Read More » -
Nkhani
Kupakula kukapitolo, JB achotsa nduna
Mtsogoleri wadziko lino Joyce Banda Lachitatu adakana kupumitsa mamulumuzana ena aboma kutsatira kupakula ndalama za boma kumene kwanyanya kulikulu la…
Read More » -
Nam yapindulanji pa Tigresses?
Bungwe la Malawi National Council of Sports tsopano layeretsa timu ya Tigresses kuti Nam ndiyo yolakwa pankhani yoti timuyi ichotsedwe…
Read More » -
Editors Pick
Nam yagwira utsi, Tigresses ipambana mlandu
Choona chavumbuluka, zenizeni zakulumana pakati pa bungwe loyang’anira zamasewero a ntchemberembaye la Netball Association of Malawi (Nam) ndi timu ya…
Read More » -
Nkhani
‘Makuponi si yankho, ingosiyani’
Ngakhale boma lili kalikiliki ndi ndondomeko ya zipangizo zotsika mtengo, mphunzitsi wa zandale Joseph Chunga komanso mkulu woona zaufulu wachibadwidwe…
Read More » -
Entertainment News
POV set to launch Ambuye Mukundimva
Everything is set. The much awaited for launch of POV’s fourth album, Ambuye Mukundimva, is here and the venue is Robins…
Read More » -
Nkhani
‘Chimanga cha 10kg tidyapo kangati’
Anthu ena akwiya m’dziko muno ndipo apempha boma kuti lisinthe ganizo lake lolamula bungwe la Admarc kuti lizigulitsa chimanga chosapitirira…
Read More » -
Nkhani
Phalombe yakonzeka kuthana ndi ngozi
Pafupifupi chaka chilichonse boma la Phalombe limakumana ndi ngozi zachilengedwe, kuthana ndi mavutowa lakhala vuto kwa zaka. Mwachitsanzo, chaka chatha…
Read More » -
Chalaka Kinnah Tom sangatole
Aganyu tidagwiritsidwa utsi titalonjezedwa ndi yemwe anali mphunzitsi wa Flames Tom Santfiet kuti Flames ikavulaza Nigeria. Nigeria idatiumbudza 2-0. Iye…
Read More » -
Nkhani
Ndale zosadula chitukuko zikhumudwitsa aMalawi
Kudula ntchito zimene adayambitsa atsogoleri akale a dziko lino kukuchititsa kuti Amalawi azingosaukirabe chifukwa ndalama zambiri zimangolowa m’madzi ntchitozo osamalizidwa.…
Read More » -
Front Page
Woman, 80, sexually abused
She was hoping to spend three hours in her maize field and return home by 10am to help her 10-year-old…
Read More » -
Nkhani
Escom isayerekeze kukweza magetsi—Banda
Kutsatira zomwe mkulu wa zachuma kukampani ya magetsi m’dziko muno ya Escom Delano Ulanje adauza wailesi ya MBC kuti bungweli…
Read More » -
Nkhani
Kanduku achotsa mfumu
Kwathina ku Mwanza pamene T/A Kanduku wachotsa gulupu Thambala komanso kulamula ena awiri kuti alipe mbuzi. Bwanamkubwa wa bomalo Gift…
Read More » -
Flames ikaluza, Tom abwerera?
Kuli nkhondo ku Calabar lero. Flames ikhala ikuphana ndi Nigeria masewero amenenso aunikire ntchito ya mphunzitsi wa Flames Tom Saintfiet.…
Read More »