-
Nkhani
Sipakala waimitsa Nyumba ya Malamulo
Sipikala waimitsa Nyumba ya Malamulo kwa sabata ziwiri kaamba ka phungu ndi ogwira ntchito ena ku nyumbayi omwe akhudzidwa ndi…
Read More » -
Nkhani
Chakwera akwanitse malonjezo—HRDC
Bungwe la Human Rights Defenders Coalition (HRDC) lati maso ake akadali otsegula n’cholinga choti boma la Tonse Alliance lisaphwanye ufulu…
Read More » -
Nkhani
Masankhidwe a nduna autsa mapiri pa chigwa
Mtsutso wabuka ndi mmene mtsogoleri wa dziko lino, Lazarus McCarthy Chakwera, wasankhira nduna za boma lake. Amalawi ena akuti sakuonapo…
Read More » -
Nkhani
Malonjezo ayamba kuoneka
Boma latsopano la Tonse Alliance layamba kukwaniritsa ena mwa malonjezo ake a panyengo ya kampeni ndipo pomwe akadaulo osiyanasiyana ayamikira…
Read More » -
Nkhani
Maudindo ayamba kuchucha m’boma
Pomwe mtsogoleri wa dziko lino yemwe wangosankhidwa kumene Lazarus Chakwera wayamba kusankha adindo m’bom, ku Nyumba ya Malamulo zinthu zasadabuzika.…
Read More » -
Editors Pick
Hopefuls in last campaign rallies
As Malawi inches towards the landmark fresh presidential election slated for Tuesday, opposition hopefuls have taken campaign to their strongholds…
Read More » -
Nkhani
Takonzeka kuvota—Amalawi
Pamene kwangotsala masiku awiri kuti Amalawi 6.8 miliyoni aponye voti yosankha mtsogoleri wa dziko lino, Amalawi ena asonyeza chidwi kuti…
Read More » -
Nkhani
Atsogoleri akwangula kampeni lero
Migwirizano ya zipani pachisankho chikudzachi zikuomba mkota wa mfundo za kampeni lero ndipo atsogoleri a m’migwirizanoyo akhala ali mbweee! kutolera…
Read More » -
National News
Lilongwe elderly receive TB Joshua’s birthday gifts
Emmanuel TV partners on Sunday donated assorted items to 30 elderly people at Kakungu Village in Traditional Authority Njewa in…
Read More » -
Nkhani
Zipani zakonzeka kusankha makomishona
Mtsogoleri wa dziko lino Peter Mutharika wauza zipani za ndale komanso nthambi yoyang’anira ogwira ntchito makhoti (Judicial Service Commission) kuti…
Read More » -
Nkhani
Covid-19 yakolera
Chiwerengero cha Amalawi amene apezeka ndi kachirombo ka coronavirus chatumphuka m’sabata ikuthayi kuchoka pa 101 kufika pa 203. Izi zachitika…
Read More » -
Nkhani
Mkokemkoke patsiku la chisankho
Zipani zotsutsa boma zalembera bwalo la milandu la Supreme Court kuti lifotokoze bwino pa za yemwe akuyenera kusankha tsiku loti…
Read More » -
Nkhani
APM alola ansah achoke
Mtsogoleri wa dziko lino Peter Mutharika dzulo wavomereza kuti wapampando wa bungwe la zisankho la Electoral Commission (MEC) Jane Ansah…
Read More » -
National News
Police, parties sign peace pact
Major political parties in the country have pledged to hold peaceful and issue-based campaign in the run-up to the fresh…
Read More » -
Nkhani
Andale agundika misonkhano, osapewa Covid-19
M’sabatayi, anthu ena 5 adapezeka ndi kachirombo ka coronavirus m’dziko muno, kuchititsa kuti chiwerengero cha anthuwo chifike pa 63. Chiopsezo…
Read More » -
Business News
Mixed fortunes for tobacco market
The AHL Group says the ongoing tobacco market’s future looks promising although high rejection rates are weighing down on the…
Read More » -
Nkhani
Mtambo walowa ndale
Yemwe adali wapampando wa gulu la Human Rights Defenders Coalition (HRDC) Timothy Mtambo wati wasintha nthabwa ndipo pano wayamba ndale…
Read More » -
Guest Spot
‘Malawians are key beneficiaries of tax’
Recently, an irate group of concerned citizens penned the Malawi Revenue Authority (MRA) as well as Officer-In-Charge for Chitipa District…
Read More » -
Nkhani
MCP, UTM asainira mgwirizano
Kudali khwimbi la anthu ku Kamuzu Institute for Sports ku Lilongwe Lachinayi pomwe zipani zotsutsa zimasayinira mgwirizano wawo motsogozedwa ndi…
Read More » -
Nkhani
Mutharika asosola nthenga atsogoleri
….asankha nduna, koma Chimunthu Banda aukana Mtsogoleri wa dziko lino Peter Mutharika sabata imene ikuthayi anali wotangwanika zedi chifukwa ndiye…
Read More »