Kusowa kwa mnyamata wa chialubino m’boma la Machinga kwavumbulutsa zinthu zoziritsa thupi. Macdonald Masambuka wa zaka 22 yemwe ankachokera m’mudzi mwa Nakawa, Mfumu…
Madzi sakudikha kuchipani cha DPP pamene mpungwepungwe wolimbirana amene adzatsogolere chipanichi ku chisankho cha 2019 wafika pa kamuthemuthe. Atsogoleri ena a chipanichi…
Apolisi a chigawo chapakati abatha msilikali wa nkhondo ndi anthu ena awiri powaganizira kuti adapezeka ndi chamba popanda chilolezo. Msilikaliyu, Alex Kanjanga wa zaka…
Ena zimbudzi zawo zikadzadza amagwetsa ndi kukumba china. Uku ndi kutha malo. Lero zinasintha chifukwa khonsolo ya Blantyre mogwirizana ndi Waste Advisers agwirizana zopopa…
Masiku ano ukatsegula wailesi kapena nyuzipepala ngakhalenso poyenda mphepepete mwa msewu ngakhalenso m’malo modikirira mabasi, uthenga omwe watenga malo ndi wa mankhwala okuza ziwalo.…
Mtolankhani wa za masewero ku wailesi ya Voice of Livingstonia (VOL) Sylvester Siloh Kapondera adakumana ndi wokondedwa wake Annie Chivunga Kalasa ali ana m’boma…
Kuchionetsero cha zaulimi cha National Agriculture Fair ku Trade Fair Grounds mumzinda wa Blantyre, Peacewell Edward Mlanga, wochokera kwa Senior Chief Somba m’boma la…
Petani Mtonga, wachiwiri kwa mkulu wa nthambi ya matenda a khansa kuchipatala cha Queen Elizabeth mumzinda wa Blantyre wati matenda akhansa akagwira mawere amatchedwa…
Ngakhale alimi ambiri a ng’ombe za mkaka amabwekera kuti akupeza phindu ku ulimiwu, Jacob Mwasinga, mlangizi wa ziweto ku Mzuzu Agricultural Development Division (Mzadd)…
Kwa zaka 12, ena mwa omwe akuwaganizira milandu yakupha akadali pa alimandi m’ndende podikira chilungamo pa milandu yoganiziridwa kuti adapha anzawo. Milanduyi,…
Sungapirire mfuu wa mbalame—wopokerezedwa bwino ngati nyimbo m’mitengo yachilengedwe m’boma la Mangochi. Nkhalango yachilengedwe ya m’mudzi mwa Chembe m’boma la Mangochi lero ndi…
Milandu yosiyanasiyana mu mzindawa Blantyre yatsika kuchoka pa 328 mu February chaka chatha kufika pa 204 mwezi omwewo chaka chino, atero apolisi. Wachiwiri…