Chichewa
-
Liwu la mafumu pa zochotsa anthu 1 miliyoni mu AIP
Mafumu apereka maganizo osiyanasiyana pa ganizo la boma lochotsa maina 1 miliyoni mu pulogalamu ya zipangizo za ulimi zotsika mtengo…
Read More » -
Boma likugwiritsa K3 biliyoni pothandiza ochotsa mimba
Dziko la Malawi likugwiritsa ntchito pafupifupi K3 biliyoni pa chaka popereka thandizo kwa amayi amene anachotsa mimba pogwiritsa ntchito njira…
Read More » -
Gogo athawa m’mudzi mwake
Abale a gogo Binwell Chabwera amene adathawitsidwa pomuganizira kuti adapha mdzukulu wake m’matsenga anenetsa kuti iwo sakufunanso kuona gogoyo. Gogo…
Read More » -
Zaka ziwiri kwa akuba pa foni
Bwalo la Nsanje Third Grade Magistrate lalamula amuna awiri kukagwira ukaidi kwa miyezi 24 atawapeza wolakwa pa mlandu woba mafoni.…
Read More » -
Alimi akhutira ndi chionetsero
Alimi ena amene afika ku chionetsero cha ulimi chimene nduna ya za malimidwe a Sam Kawale adatsegulira dzulo mu mzinda…
Read More » -
Aphungu akwangula zokambirana
Pamene aphungu a Nyumba ya Malamulo amayembekezeka kukwangula zokambirana zawo dzulo, mkulu wa bungwe loona za ufulu wa anthu la…
Read More » -
Maneb itulutsa maina aophunzira 10 okhoza kwambiri
Bungwe la za mayeso la Malawi National Examinations Board (Maneb) latulutsa mndandanda wa ophunzira 10 amene achita bwino kwambiri pa…
Read More » -
Ng’anga zaithina itakanika kudzutsa munthu wakufa
Ng’anga ina ku Balaka yapereka chindapusa cha K90 000 kupewa kukaseweza miyezi 15 imene adamugamula atapezeka wolakwa pa mlandu woti…
Read More » -
Misika ya Admarc siyitsegulidwa msanga
Nduna ya za malimidwe a Sam Kawale ati kampani yogula mbewu ya Admarc siyitsegulidwa kuti iyambe kugula mbewu pokhapokha anthu…
Read More » -
Zaka 59 pa ufulu tapindulanji
Kadaulo pa ndale a George Phiri ati palibe chifukwa chomveka choti dziko la Malawi lizikondwerera ufulu wodziimirira palokha chifukwa m’zambiri…
Read More » -
Aphana pachibale kaamba ka malo
Apolisi m’boma la Lilongwe amanga abambo atatu a banja limodzi powaganizira kuti adapha mbale wawo polimbirana malo m’mudzi mwa Maliseni…
Read More » -
Loans board struggles to recover K16bn
The Higher Education Student’s Loans and Grants Board (HESLGB) says it is struggling to recover K16 billion from its beneficiaries.…
Read More » -
Mlandu wa a Bushiri ukhalako pa Julayi 10
Mlandu wa a Pulofeti Shepherd Bushiri ndi akazi awo a Mary unalephereka kuyamba Lachiwiri kaamba ka kusagwirizana kumene kunalipo pakati…
Read More » -
Centre turns to parley on rising food costs
The Centre for Social Concern (CfSC) has urged members of Parliament to discuss and pass the Right to Food Bill…
Read More » -
Chomwe aimitsira mlandu wa a muluzi chidziwika lolemba
Mkulu wa bungwe loyendetsa milandu la Director of Public Prosecutions (DPP) a Masauko Chamkakala akuyembekeza kuuza Amalawi chifukwa chomwe aimitsira…
Read More » -
MEC yakonzeka kulanga osokoneza
Chisankho cha 2025 chikhoza kuzakhala umboni wa ulamuliro weniweni wa demokalase ngati bungwe la Malawi Electoral Commission (MEC) lizatsate malamulo…
Read More » -
Umitsani chimanga mokwanira ngakhale mvula ikugwabe
Adathawitsa chimanga m’munda chisadaumitsitse kuopetsa kuti chionongeka ndi mvula imene ikupitirirabe kugwa m’dziko muno komanso akuba amene akuba mopanda chisoni.…
Read More » -
Azengedwa mlandu wopha mkazi wake ku mangalande
Nyuzipepala zikuluzikulu za ku Mangalande Lachisanu zidadzala ndi nkhani ya bambo wina wa ku Malawi amene akumuganizira kuti adabaya ndi…
Read More » -
Mpungwepungwe ku msika wa fodya
Kudali mpungwepungwe kumsika wa fodya wa Kanengo mumzinda wa Lilongwe pomwe alimi adakwiya ndi mitengo ya fodya ndipo adauza ngakhale…
Read More » -
Mneneri akhala osadya komanso kumwa masiku 40
Mneneri Ellason Zande akuti anafa n’kudzukanso pomwe anasala kudya kwa masiku 40, Mulungu atawaonekera. A Zande omwe akuchita utumiki wawo…
Read More »