-
‘Padali pachiwaya cha tchipisi’
“Adayezetsa tchipisi cha K150, ine ndidamuonjezera kuti agule cha K200.” Mmenemo ndi momwe zidayambira kuti Henry Mbinga akumane ndi Chimwemwe…
Read More » -
Chichewa
Chigodola chavuta ku Nsanje
Ng’ombe 70 m’boma la Nsanje zikutsalima, pamene 65 000 kumeneko zili pachiopsezo chotenga matenda a chigodola amene abonga m’bomalo.…
Read More » -
Chichewa
Chilala chavuta maboma ambiri
Nduna ya zamalimidwe ndi chitukuko cha madzi, Dr Allan Chiyembekeza, wati pakhala msonkhano wounikira momwe ng’amba yakhudzira anthu makamaka m’chigawo…
Read More » -
Chichewa
Obzala nthawi ya maliro athothedwa
Thambo likagwa m’mudzi, aliyense amayenera ayandikire chifupi ndi siwa kuti athandizane nthawi ya zolemetsayi. Kudagwa zovuta m’mudzi mwa Mazale kwa…
Read More » -
National Sports
Chiyembekeza launches trophy
Minister of Agriculture, Irrigation and Water Development Allan Chiyembekeza on Sunday launched a K5 million (about $7 174) league in…
Read More » -
Chichewa
Zampira zenizeni ndi CJ Banda
John CJ Banda ndi kaputeni wa Blue Eagles, komanso ndi katundu wofunika ku Flames. Iye wapeza mwayi wokasewera ku…
Read More » -
Nkhani
Adakumana bwanji m’chakacho?
Ankadzapepesa maliro a mkazi wanga’ Ukwati ndi chinthu chabwino, ndipo Mulungu amasangalala nacho. Chaka cha 2015 Mulungu adadalitsa ena ndi…
Read More » -
Nkhani
Mudalinji m’chakachi?
Ma alubino aona zakuda Mpotopola ku Joni, Amalawi 3 200 athothedwa Anthu 106 afa ndi madzi osefukira Tili m’chaka…
Read More » -
Nkhani
Tidacheza nawo bwanji?
M’chaka cha 2015 tamva zikhulupiriro, miyambo komanso mbiri zosiyanasiyana za maderanso osiyana. Lero BOBBY KABANGO akutibweretsera macheza ochepa amene nkhani…
Read More » -
Chichewa
Mabungwe athotha galu wakuda ku MJ
Anthu m’boma la Mulanje omwe adakhudzidwa ndi njala kaamba ka ngozi za kusefukira kwa madzi komanso chilala kumayambiriro a…
Read More » -
Nkhani
‘Kupitakufa? Mbiri yakale imeneyo!’
Matenda a HIV/Edzi asokoneza miyambo ina monga mwambo wa kupitakufa, womwe umapereka mphamvu kwa ‘fisi’ kuti akakonze maliro pocheza ndi…
Read More » -
Chichewa
Ophunzira asanu anjatidwa ku Nkhotakota
Apolisi Lolemba adamanga ophunzira asanu a sukulu ziwiri za m’boma la Nkhotakota ndi kuwatsegulira mlandu wofuna kudzetsa chisokonezo. Mneneri…
Read More » -
Chichewa
Chilango chowawa kwa wogulitsa nyama ya galu
Bwalo la majisitireti la Balaka lapereka chilango chowawitsa kwa mkulu amene wakhala akugulitsa nyama yagalu kwa zaka 14. Pamene…
Read More » -
Chichewa
Nthula: Abambo ofooka kuchipinda achangamuke
Akuti abambo ena amafooka pamene akucheza ndi akazi awo chifukwa cha zina zomwe zimasowekera pamene machezawa ali mkati. Ichi nchifukwa…
Read More » -
National News
Neno communities receive K109m to fight deforestation
Communities in Neno have every reason to stop environmental degradation and restore land as government through the Shire River…
Read More » -
Chichewa
Osabweza ngongole ya Mardef ali m’madzi
Anthu amene sadabweze ngongole ya Malawi Enterprise Development Fund (Mardef) ali m’madzi pamene ayamba kuona zakuda. Ngongole ya Mardef…
Read More » -
Chichewa
Afa atamwa bibida wosadyera
Mneneri wa polisi ya Nkhotakota Williams Kaponda watsimikiza kuti bambo wina kumeneko wakabzala chinangwa atapapira mowa osadyera. Kaponda adati…
Read More » -
Chichewa
‘Ankadzapepesa maliro a mkazi wanga’
Imfa ya mkazi kapena mwamuna wako si mathero amoyo. Mulungu amakoza njira ina kuti akupepese bwinobwino ndipo uyiwale zakale.…
Read More » -
Chichewa
Alimi konzekani kukolola madzi
Mvula ya masiku ano ndi yanjomba. Zikatere mlimi amayenera kuchenjera kuti aphulepo kanthu ngakhale mvula itadula msanga. Ichi nchifukwa chake…
Read More » -
Chichewa
Kusamala anapiye a mikolongwe
Amati nkhuku ndi dzira, kusonyeza kuti ngati susamala dzira ndiye kuti udzalandira nkhuku za matenda zomwe sizichedwa kufa. Komanso kupanda…
Read More »