-
Dz Young Soccer, ‘Mighty’ adutsa
Chikho cha Standard Bank chayamba ndi moto pamene matimu a asirikali a Kamuzu Barracks ndi Mafco FC aona msana wa…
Read More » -
Nkhani
Mwambo woliza mfuti pamaliro Achingoni
Mfumu Yachingoni ikagona, pamaliropo amaomba mfuti thupi la mfumuyo lilowe m’manda. Mwezi wathawu, kudachitika maliro a T/A Bvumbwe m’boma la…
Read More » -
Nkhani
Umhlangano wa Maseko Ngoni lero
Kutentha masanawa kumanda kwa Gomani kwa Nkolimbo m’boma la Ntcheu pamene Angoni a m’maiko monga Zambia, Mozambique, Tanzania, South…
Read More » -
Nkhani
Moto buu! Ku Swaziland
Kochi wa timu ya dziko lino ya Malawi Flames, Ernest Mtawali, wati timu yake yakonzeka kuonetsa zakuda timu ya Swaziland…
Read More » -
Chichewa
Katundu wakwera udyo, atero anthu
Amalawi akonzekere kulira chifukwa cha kukwera udyo kwa mitengo ya zakudya ndi katundu wina komwe kwachitika kuyambira mwezi wa…
Read More » -
Chill
Umhlangano wa Maseko tomorrow
As they do around this time of the year, it is time for Maseko Ngonis to take their spot…
Read More » -
Chichewa
Wopezeka’ ndi yunifomu ya polisi anjatidwa
Apolisi ku Zomba akusunga m’chitolokosi bambo wa zaka 25 pomuganizira mlandu wopezeka ndi yunifomu ya polisi komanso mfuti popanda…
Read More » -
Chichewa
Wobwerera lili pululu amwaliranso ku zomba
ZImene zachitika m’mudzi mwa Makoloni kwa T/A Mwambo ku Zomba masiku apitawa n’zoda mutu. Mayi wa zaka 28 amene…
Read More » -
Chichewa
Zefinati Alick: Kadaulo posema ziboliboli
Aluso ndi onse koma luso losema ziboliboli si lachibwana, limafunika khama komanso munthu wolimba mtima. Pa Golomoti m’boma la Dedza…
Read More » -
Thambo lagwa kwa Bvumbwe
Thambo lagwa! Yagona ngwenyama, mfumu Yachingoni kwa Bvumbwe m’boma la Thyolo, komwe anthu ochokera m’maboma osiyanasiyana akhamukire m’mudzi mwa Makungwa…
Read More » -
Nkhani
Msika wa osewera watentha
Pamene matimu ali kopumira kukonzekera ndime yachiwiri ya 2015 TNM Super League, msika wa osewera wafika potentha pamene matimu ali…
Read More » -
Nkhani
Samalani: Kwabuka matenda a chimanga
…Boma liletsa kugula mbewuyi m’maiko akunja okhudzidwa Chilinganizo cha boma choletsa kugula chimanga m’maiko a South Sudan, Uganda, Kenya, DR…
Read More » -
Chichewa
Amangidwa kaamba kobisa khanda
Pamene amayi ena akukangana ndi amuna awo m’midzimu kufuna nsalu yalekaleka, amayi ena ndi pamene mwayi woterewu akumauseweretsa n’kumataya ana…
Read More » -
Chichewa
Amati aukitsa wakufa koma athera m’zingwe
Mudali fumbi m’mudzi mwa Mpheziwa kwa T/A Kasumbu m’boma la Dedza posachedwapa pamene khwimbi la anthu lidakhamukira m’mudzimo kukaonerera ntchito…
Read More » -
Nkhani
Kwagwedezeka ku PP
Potsata mawu a mtsogoleri wakale wa dziko lino Bakili Muluzi onena kuti chipani cha MCP “chatha ngati makatani”, zikuoneka kuti…
Read More » -
Nkhani
Sakumvanabe pa nkhani za ufumu
Pali kusamvanabe pakati pa unduna wa maboma aang’ono ndi mafumu a m’mizinda amene boma, kudzera mu undunawu, lidawalembera kalata yowadziwitsa…
Read More » -
Chichewa
Amukwidzinga Pachinkhoswe
Amati mbuzi ikakondwa amalonda ali pafupi. N’zoonadi, Ili lidali tsiku lachisangalalo ndipo kudali kuvina, amayi nthungululu zili pakamwa. Anthu adabwera…
Read More » -
Mwambo wogwetsa simba
Sukulu zatsekera ndipo zikatere m’maboma ambiri makolo ali kalikiriki kukonzekera kuti ana awo apite kusimba kukavinidwa. Kumenekotu kumakhala uphungu kuti…
Read More » -
Nkhani
Pepani Ng’onamo, Chirwa
Kudali ntchito ku FAM pamene amafuna kochi wa timu ya fuko ya Flames. Eddie Ng’onamo, Nsanzurwimo Ramadhan, Ernest Mtawali…
Read More » -
Nkhani
Utsi ku Nam pamene ma Queens anyamuka
Utsi ukufukabe ku bungwe loyendetsa masewero a ntchemberembaye la Netball Association of Malawi (NAM) kaamba kosemphana zochita pakati pa mphunzitsi…
Read More »