Tuesday, September 26, 2023
  • About Us
  • ImagiNATION
  • Rate Card
  • Contact Us
The Nation Online
Advertisement
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Enation
No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Enation
No Result
View All Result
No Result
View All Result
Home Chichewa Nkhani

Mswati akhale chitsanzo kwa achinyamata

by Johnny Kasalika
11/08/2012
in Nkhani
1 min read
0
Share on FacebookShare on TwitterShare on WhatsAppShare on LinkedinLinkedinShare via Email

Pulezidenti Joyce Banda wati mfumu yachingoni yomwe angoidzoza kumene, Mswati Kanjedza Gomani yachisanu ikhale chitsanzo kwa achinyamata.

Banda amalankhula izi Lamulungu pa 5 Ogasiti pomwe adali mlendo wolemekezeka ku mwabowo ku Lizulu m’boma la Ntcheu.

Mwazina Banda adapempha anthu andale kuti asasokoneze mfumuyi, yomwe ndi ya zaka 17.

“Tithandize mfumu yathu kuti igwire bwino ntchito. Fumu ikhale yachilungamo, yodziwa kuweruza milandu; amati milandu sagula ndi chipanda cha mowa.

“Komanso, ngati boma, ndife osangalala kukhala ndi mfumu yachinyamata ngati imeneyi chifukwa ikhala chitsanzo chabwino kwa achinyamata.

‘Zomwe izichita mfumuyi achinyamata adzitengera iyo,” adatero Banda.

Mswati Gomani walowa ufumuwo kutsatira imfa ya bambo ake, Willard Kanjedza Gomani yachinayi yomwe idamwalira mwezi wa Sepitembala mu 2009.

Pamwambowo, kudabwera akuluakulu andale komanso amabungwe.

Nayo mfumu yaikulu ya angoni m’dziko la Mozambique, T/A Zimtambira, idali nawo pamwambowo.

Previous Post

Ngumi brings night of fights

Next Post

Fight for supremacy at Local Govt Ministry

Related Posts

Nkhani

 Liwu la mafumu pa zochotsa anthu 1 miliyoni mu AIP

September 23, 2023
Nkhani

Boma likugwiritsa K3 biliyoni pothandiza ochotsa mimba

September 23, 2023
Gogo Chabwera
Nkhani

Gogo athawa m’mudzi mwake

September 17, 2023
Next Post
The Nation Online Fight for supremacy at Local Govt Ministry

Fight for supremacy at Local Govt Ministry

Opinions and Columns

My Turn

Resolve DStv spat amicably

September 25, 2023
People’s Tribunal

Time for politicians to memorise the myth of Sisyphus

September 24, 2023
Big Man Wamkulu

I hear he is engaged to somebody

September 24, 2023
Musings on Corruption

Is ‘God-fearing’just a façade?

September 24, 2023

Trending Stories

  • Kept report under wraps: Chakwera

    Inside ‘hidden’ Reforms report

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Mysterious animal injures 9 people

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • RBM wants suspension of judgement in ICT deal

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Just kill me—cries Cashgate convict

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Strange illness scare forces school to close

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Values
  • Our Philosophy
  • Editorial policy
  • Advertising Policy
  • Code of Conduct
  • Plagiarism disclaimer
  • Disclaimer
  • Privacy Policy
  • Terms of use

© 2023 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Enation

© 2020 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

This website uses cookies. By continuing to use this website you are giving consent to cookies being used. Visit our Privacy and Cookie Policy.