Nkhani
-
Dikirani kauniuni wachiwiri wa mbewu
Unduna wa za malimidwe wati anthu asathyolere khosi zotsatira za kauniuni woyamba wa mbewu chifukwa kauniyo sadalingalire za ng’amba yomwe…
Read More » -
Sakufuna awakanize kuima
Mamembala ena a chipani cha Malawi Congress (MCP) akutsutsana ndi maganizo amene komiti yaikulu ya chipanicho (NEC) idamanga kumsonkhano wake.…
Read More » -
Anjata wofuna kugulitsa mwana wake
A Chimwemwe Zololo atha masiku 6 m’chitokosi cha apolisi ku Zomba powaganizira kuti amafuna kugulitsa mwana wompeza. A Zololo akuyembekezereka…
Read More » -
Wa zaka 15 amuganizira kupha mchemwali wa 26
Mwana wa zaka 15 ali m’manja mwa apolisi ku Mangochi pomuganizira kuti adazimitsa mchemwali wake wa zaka 26 pa mkangano…
Read More » -
Ululu podula cha unzika
Walira mvula waliranso matope. Anthu amene amalakalaka atapeza chiphaso cha unzika mwayi wawagwera koma ayenera akhetse thukuta kuti izi zitheke.…
Read More » -
A Chakwera alephera kukwaniritsa lamulo lawo lomwe
Akatswiri pa nkhani za chuma ndi ufulu wa anthu adzudzula mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera kaamba kolephera kukwaniritsa…
Read More » -
Aonjezera aphungu
Bungwe loyendetsa zisankho la Malawi Electoral Commission (MEC) latsutsa mphekesera yoti layamba laimika kaye chilinganizo choonjezera madera a aphungu pa…
Read More » -
Msungwana adakokera boma kukhoti
Chaka cha 2023 chikupita ndi nkhani zake, imodzi mwa nkhani zimene zidayala nthenje ndi ya msungwana wa zaka 14 yemwe…
Read More » -
Mfumukazi ichereza mayi wobereka ana 5 pa kamodzi
Mkazi wa Inkosi ya Makhosi Gomani V, Inkosikati Rishaladza Khanyisa Gomani wati kuchuluka kwa mimba za ana achichepere kukukolezera kusachita…
Read More » -
Owaganizira kupha anthu 4 amangidwa
Apolisi amanga anthu 6 omwe akuwaganizira kuti adatengera lamulo m’manja mwawo potengapo gawo pa kuphedwa kwa abambo 4 omwe amaganiziridwa…
Read More » -
Akuti mtima mmalo, chitetezo chilipo pa zisangalalo
Nduna ya za chitetezo cha m’dziko a Ken Zikhale Ng’oma ati unduna wawo wakhwimitsa chitetezo m’nyengo ya zisangalalo za Khrisimasi…
Read More » -
DPP idyera Khrisimasi m’khoti
Woweruza ku bwalo la milandu lalikulu ku Lilongwe a Justice Howard Pemba ati adzapereka chigamulo chawo pa 26 December 2023…
Read More » -
Mchitidwe wogona ndi ana ukukula kwambiri
Pamene bwalo lina ku Zomba m’sabata yangothayi lidagamula kuti mphunzitsi wina ndi wosalakwa pa mlandu wogwiririra mwana wophunzira pasukulu ya…
Read More » -
Ziphaso zitheka pofika 2025
Nduna ya za chitetezo cha m’dziko a Ken Zikhale Ng’oma ati pofika m’chaka cha 2025 pomwe Amalawi adzaponye voti ya…
Read More » -
Kwafa bulu ku DPP
Mtsogoleri wa chipani cha Democratic Progressive (DPP) a Peter Mutharika wauza mamembala omwe sakumumvera m’chipanicho kuti achoke asaononge chipani. A…
Read More » -
Mfumu yadzikhweza ndi za fetereza wa AIP
Amfumu a Chidzalo a zaka 71 omwe dzina lawo ndi a Moffat Lamulani Mlenga a m’boma la Dowa adzikhweza pothawa…
Read More » -
Amanga 10 pa mkangano wa ufumu
Apolisi ku Ntchisi amanga anthu 10 a m’mudzi mwa Kanyenda kwa T/A Kalumo potsatira mkangano wa ufumu pakati pa a…
Read More » -
Mitala iphetsa
Mayi wa zaka 19 wadzipha ku Kasungu atazindikira kuti mwamuna yemwe adakwatirana naye pokhulupirira kuti banja lake loyamba lidatha ndi…
Read More » -
Chiyembekezo chakwera ndi mawu a Chakwera
Pakati pa usiku wa Lachitatu sabata yatha, ndalama ya kwacha idatsika mphamvu ndi K44 pa K100 iliyonse. Izi zachititsa kuti…
Read More » -
chiwanda chophana chavuta
Chiwanda chachilendo chophana m’mabanja chalowerera moti mwezi umodzi okha, bambo wina ku Zomba adapha mkazi wake, banja lina ku Chiradzulu…
Read More »