Ena apeza golide pa vuto la mafuta
Pomwe Amalawi akulira ndi vuto la kusowa kwa mafuta a galimoto lomwe laimitsa ntchito zambiri makamaka zodalira mafutawo, anthu ena...
Pomwe Amalawi akulira ndi vuto la kusowa kwa mafuta a galimoto lomwe laimitsa ntchito zambiri makamaka zodalira mafutawo, anthu ena...
Pomwe aphungu a ku Nyumba ya Malamulo akuyamba mkumano wawo wounika bajeti ya 2022-2023 pa 14 November 2022, Amalawi ati...
Makomiti a Nyumba ya Malamulo omwe akuunika momwe feteleza wa AIP adagulidwira kuti ndalama zina zokwana K750 miliyoni zisokonekere aluma...
Mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera achenjeza nduna zawo kuti yense osatha ntchito yake achotsedwa paudindo wake chifukwa nduna...
Apolisi m’boma la Lilongwe, akusaka mnyamata wa zaka 17 pomuganizira kuti anamenya ndi kupha bambo ake a zaka 33 chifukwa...
Ndi K12 000 yokha amagula feteleza wa mkodzo wokwana malita 20 ndi kusungunula n’kuthira m’munda. Akatero mlimiyo a Winston Devie...
Bwalo la milandu la majisitileti ku Kasungu Lachitatu lidagamula bambo wa zaka 26, a Geoffrey Kwenda kuti akaseweze kundende zaka...
Mitima ya Amalawi ili dyokodyoko kudikira zomwe mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera abweretse pochoka kumsonkhano wa atsogoleri a...
Bungwe la ogula katundu la Consumers Association of Malawi (Cama) lati boma lalakwitsa kuimitsa ntchito za kampani yake ya Admarc...
Zipani zina za ndale m’dziko muno zati sizikukhutira ndi momwe malire atsopano a madera a aphungu ponena kuti maganizo awo...
Boma ladandaula kuti ndalama zochuluka za bajeti ya zaumoyo zikulowa pothandiza mavuto opeweka monga ngozi zapamsewu zokhudza akabaza a njinga...
Patrick Mwaungulu ndi mnyamata wachichepere koma wa luso lalikulu pokankha chikopa ku timu ya Nyasa Big Bullets. Mwaungulu anasankhidwa ngati...
Mtsogoleri wa chipani cha UTM a Saulos Chilima womwenso ndi wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino dzulo aulula zomwe adagwirizana...
Mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera ati kuyambira Lachiwiri lapitali adasiya kupereka ntchito kwa wachiwiri wawo a Saulos Chilima...
Mayi wina yemwe ndi mlembi kunthambi yoyang’anira za umoyo pakhonsolo ya mzinda wa Mzuzu, anadabwitsa anthu masiku apitawa pomwe anasamukira...
Anthu a m’dera la Mchenga-utuba mumzinda wa Mzuzu akukhala mwa mantha woimba wina wodziwika m’deralo atabedwa sabata yatha. Woimbayu Dickson...
Nthambi yoona za ngozi zogwa mwadzidzidzi ya DoDMA yatolera K34.8 biliyoni ya ngozi zogwa mwadzidzidzi koma ndalamazo n’zochepa poyerekeza ndi...
Abambo ena 8 adabwitsa anthu ku Chibavi, mumzinda wa Mzuzu atapezeka ndi yunifomu zapolisi. Zovalazi ndi monga zigoba zovala panthawi...
Ntchito zambiri m’dziko muno zasokonekera kapena kuima kumene potsatira kusowa kwa ndalama zakunja zomwe zimagwiritsidwa ntchito poitanitsa katundu. Umboni wafika...
Nthambi ya zandende m’dziko muno yaimika kaye pantchito woyang’anira ndende Emmanuel Chiganda, yemwe mkaidi amene adapezeka ndi foni ziwiri m’mimba...