Chichewa
-
Milandu ya ‘kashigeti’ yayamba kusongola
Nkhani zakubedwa kwa ndalama m’boma ya kachigeti tsopano yayamba koneka mutu wake. Padakali ano, anthu atatu apezeka olakwa pamlandu owaganizira…
Read More » -
Mafumu akwiya ndi kufukula manda
Chati delu chaopsa mlenje. Kubedwa kwa matupi a makanda ozizira pamene angoyikidwa kumene kwazwetetsa mafumu. Mchitidwewu wakula ku Chilobwe mumzinda…
Read More » -
Boon for businesses on regional payment
Malawian businesses could improve on efficiency and reduce transactional costs on foreign correspondent banking charges by using regional real-time payment…
Read More » -
PCL graduates 18 in leadership
Conglomerate Press Corporation Limited (PCL) on Tuesday graduated 18 of its managers in a leadership development programme at a ceremony…
Read More » -
Illovo donates K1m to Karonga Museum
Illovo Sugar (Malawi) Limited has donated K1 million to Karonga Cultural and Museum Centre to support the rehabilitation of the…
Read More » -
Masauko Chipembere phase III starts end November
Blantyre City Council (BCC) has said phase III of the Masauko Chipembere Highway project is set to resume at the…
Read More » -
Olumala asaiwalidwe, Fedoma yatero
Makhansala awapempha kuti akamakonza ndondomeko zachitukuko aziganiziranso olumala omwe amasalidwa. Mkulu wa mapologalamu ku mgwirizano wa mabungwe oona za olumala…
Read More » -
Waganyu: Kulibe mipira yokonzekera zoona?
Bungwe la FAM laletsa anyamata a Flames kuti asachite zokonzekera chifukwa ndalama palibe. Pofika dzulo zidali zisadadziwike ngati Malawi isewere…
Read More » -
Illovo Cycling returns
The annual Illovo Classic Cycling Race returns to action at Hill View in Blantyre this Saturday with an improved sponsorship…
Read More » -
Amalawi 9.5 miliyoni angakhale akhungu
Bungwe logwira ntchito zopulumutsa anthu ku vuto la khungu dziko lonse la pansi la Sight Savers lati Amalawi 9.5 miliyoni…
Read More » -
Kusamvetsetsana kwabuka ku Mwanza
Kusamvetsetsana kwabuka pakati pa anthu a ku Mphete m’boma la Mwanza ndi ofesi ya DC wa bomali chifukwa cha nyumba…
Read More » -
Waganyu: Nzeru zayekha adaviyika Flames
Akulu adati nzeru zayekha adaviyika nsima m’madzi. Lero tikuti nzeru zayekha adaviyika Flames m’madzi. Zidachitika ku Algeria sindizo, timu yathu…
Read More » -
Trade unions back tenants’ petition to APM
A local trade union and social justice groups as well as international observers have backed the Tobacco and Allied Workers’…
Read More » -
Mawu supports non-fiction writers
The Malawi Writer Union (Mawu) has thrown its weight behind the establishment of a separate writers’ body, the Malawi Union…
Read More » -
Kugawana ulamuliro kungatheke ku MW?
Pomwe mtsutso ukupitirira pa maganizo woti atsogoleri a dziko lino azigawana zigawo zozilamulira watenga malo, nduna ya zofalitsa nkhani Kondwani…
Read More » -
This kind of justice sulks
October 7, 2014 Anybody who stole taxpayers’ money under the infamous Cashgate should now stop worrying themselves to death for…
Read More » -
Okhala kumalire ku Phalombe akulira
Anthu ena ku Phalombe adandaula ndi nkhanza zimene amachitiridwa akapita m’dziko la Mozambique ndiponso ndi chiwerengero cha ana obedwa m’bomalo.…
Read More » -
Lake of Stars back bigger, but…
Good people, every death in the name of entertainment is lamentable and needless. This is why I sensed nothing bigger…
Read More » -
Makhansala ayamba mopendama
Pamene pangodutsa miyezi 4 chisankhireni makhansala, anthu ena akudandaula kuti makhansalawa ayamba kubisala ndipo sakuwayendera kuti amve mavuto awo. Mwachitsanzo,…
Read More » -
Wa ganyu: Sesani m’nyumba
Aganyu tadza pamaso panu bwana Kondi Msungama kaamba ka mpungwepungwe omwe wamanga nthenje kutimu ya Big Bullets. Mphongo zikutsanzika kuti…
Read More »