Friday, August 19, 2022
  • About Us
  • ImagiNATION
  • Rate Card
  • Contact Us
The Nation Online
Advertisement
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
No Result
View All Result
Home Chichewa

Wopezeka’ ndi yunifomu ya polisi anjatidwa

by Bobby Kabango
30/08/2015
in Chichewa
1 min read
0
Share on FacebookShare on TwitterShare on WhatsAppShare on LinkedinLinkedinShare via Email

 

Apolisi ku Zomba akusunga m’chitolokosi bambo wa zaka 25 pomuganizira mlandu wopezeka ndi yunifomu ya polisi komanso mfuti popanda chilolezo.

Nyaude: Tidadabwa ndi zochitika zake
Nyaude: Tidadabwa ndi zochitika zake

Mneneri wa polisi kuchigawo chakummawa, Thomeck Nyaude, watsimikizira za nkhaniyi ponena kuti adanjata Clement Mawerenga wa m’mudzi mwa Katete, T/A Malemia pamsika wa Songani.

“Tidadabwa ndi zochitika za mkuluyu ndipo titamuyandikira tidaona kuti sadali wapolisi ngakhale adapezeka ndi katunduyo. Adali ndi malaya komanso mabuluku a polisi 12 kuphatikizapo mfuti,” adatero Nyaude.

Kuchigawo chakummawa komweko, apolisi m’boma la Machinga atsekera amuna anayi powaganizira mlandu woba katundu wa K3.7 miliyoni.

Nyaude adati anthuwa akuwaganizira kuti adaba mapaipi 244 a madzi ndi zipangizo zina kwa White Mbalame, wa m’mudzi mwa Kawinga, kwa T/A Kawinga m’bomalo.

Nyaude adati amene akuwaganizira za mlanduwu ndi Madalitso Wasi, Andrew Amin, White Samson ndi Christopher Chapita.

“Tikuwaganizira kuti adapalamula mlanduwu mu November 2013. Titangowamanga, tapeza mapaipi 160,” adatero mneneriyu.

Oganiziridwawa onse akuchokera kwa T/A Mlomba m’bomalo.n

 

Previous Post

Wobwerera lili pululu amwaliranso ku zomba

Next Post

The donkey and purchaser

Related Posts

Patrick sakubwerera mmbuyo pa chikopa
Nkhani

Patrick Mwaungulu ndi katakwe pokankha chikopa

July 24, 2022
Chilima: Change the mindset toward development
Nkhani

A Chilima abwera poyera

July 1, 2022
Nkhani

Achilima awachepetsera mphamvu zaulamuliro

June 24, 2022
Next Post

The donkey and purchaser

Opinions and Columns

Business Unpacked

Why public debt should worry every patriotic Malawian

August 18, 2022
Rise and Shine

How to triumph in interviews

August 18, 2022
My Turn

Making briquettes at Malasha

August 15, 2022
Candid Talk

When parents demand more

August 14, 2022

Malawi-Music.com Top10

Trending Stories

  • Court snubs tenants on govt houses

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • ‘Blantyre derby could have fetched more’

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Why graft cases stall

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • World Bank protests K14bn ICT contract

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Govt appoints university working committee

    0 shares
    Share 0 Tweet 0

  • Values
  • Our Philosophy
  • Editorial policy
  • Advertising Policy
  • Code of Conduct
  • Plagiarism disclaimer
  • Disclaimer
  • Privacy Policy
  • Terms of use

© 2022 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation

© 2020 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

This website uses cookies. By continuing to use this website you are giving consent to cookies being used. Visit our Privacy and Cookie Policy.