-
Nkhani
Apempha achinyamata asunge bata
Pamene dziko lino likukonzekera kuponya mavoti Lachiwiri likudzali, wapampando wa bungwe la Machinga District Youth Network a Mphatso Chikaonda apempha…
Read More » -
Nkhani
Lorani mtendere ulamulire
Kampeni ikutha mawa. Atsogoleri atambasula mfundo zawo za chitukuko zomwe zili m’manifesto. Nawo mabungwe a Oxfam ndi Women Legal Resource…
Read More » -
Nkhani
Mabungwe akufuna malamulo okhudza AI
Mabungwe a Centre for Human Rights and Rehabilitation (CHRR) ndi Malawi Human Rights Commission (MHRC) apempha boma kuti liunikenso malamulo…
Read More » -
Nkhani
Zikhalidwe zikukhomerera amayi
Wapampando wa Engalaweni Women Group a Mervis Mvula akuti zikhalidwe, zikhulupiriro ndi umphawi ndizo zikulepheretsa amayi ambiri kulowa ndale. A…
Read More » -
Nkhani
Dolo ndi ndani mu chipeta ichi?
Pamene kwatsala masiku atatu okha kuti nzika za dziko lino zivote, atsogoleri omwe akuimira pa mipando ya upulezidenti, uphungu wa…
Read More » -
Asafuna kusaina pangano osamuvotera
Kampeni ya zisankho za mtsogoleri wa dziko lino, aphungu a Nyumba ya Malamulo ndi makhansala yafika pa mwana wakana phala.…
Read More » -
Chichewa
Achinyamata sakufooka, sakubwerera mmbuyo
Achinyamata, omwe adzapikitsana nawo pa zisankho za makhansala ndi a phungu a Nyumba ya Malamulo pa 16 Sepitembala, maso awo…
Read More » -
Chichewa
A Joyce Banda ndi amayi okhawo omwe akufuna kudzapikisana nawo
Pofika dzuro m’mawa, atsogoleri 14 ndiwo anatenga makalata kuchokera ku bungwe la Malawi Electoral Commission (MEC) ofuna kudzapikisana nawo pa…
Read More » -
National News
MCP, DPP ilipirira amayi osowa ku bungwe la MEC
Zipani za Malawi Congress Party (MCP) ndi Democratic Progressive Party (DPP) zilipirira amayi omwe achite bwino pa zisankho za chipulula,…
Read More » -
Women yakhazikitsa manifesito
Akatswiri omenyera ufulu wa amayi akuti manifesito ya amayi ndi chida cha mphamvu chosinthira moyo wawo pa ndale m’dziko muno.…
Read More »