-
Nkhani
Mitsinje isefukiranso chaka chino—azanyengo
Nthambi yopima zanyengo ya mdziko muno ya Department of Climate Change and Meteorological Services (DCCMS) yati chaka chino kukhala kusefukira…
Read More » -
Nkhani
Osiyidwa pachilumba cha Ruo alira koto!
Ndi 5 koloko mmawa, Belita Zakeyu wa m’mudzi mwa Manthenga kwa T/A Mlolo m’boma la Nsanje wafika kale m’manda a…
Read More » -
Nkhani
A Escom adziwe kuti takwiya—Kapito
Si zachilendonso, nyimbo yomwe aliyense akuimba ndi kuzimazima kwa magetsi. Mmalo mopereka magetsi tsiku lililonse monga anenera, ayamba kupereka mdima…
Read More » -
Nkhani
Kuthimathima kwa magetsi kwakhudzanso akumidzi
Ndi Lolemba mmbandakucha wa pa 12 September, nthawi yangokwana kumene 4 koloko koma magetsi azima kale m’boma la Mulanje. Chiyembekezo…
Read More » -
Nkhani
Gulewamkulu ndi mankhwala
Matenda akagwa pakhomo, makolo amakhala ndi njira zochuluka zothetsera matendawo malinga ndi zikhulupiriro zawo. Ena okhulupirira gulewamkulu akuti ngati m’thupi…
Read More » -
Nkhani
Siteshoni ya Nkaya ifewetsa maulendo
Gawo lachiwiri lomanga siteshoni ya sitima ya Nkaya m’boma la Balaka layamba ndipo ntchitoyi ikuyembekezeka kutha mu November chaka chino.…
Read More » -
Akwiya ndi bungwe la MEC
Mpungwepungwe umene ukuchitika kubungwe loyendetsa zisankho la Malawi Electoral Commission (MEC) wakwiyitsa zipani zotsutsa komanso omenyera ufulu omwe apempha kuti…
Read More » -
Nkhani
MEC igwira njakata pa zisankho zapadera
Zinthu sizikuyenda kubungwe loyendetsa zisankho la Malawi Electoral Commission (MEC) komwe tsogolo la zisankho zapadera silikudziwika. Lachitatu lapitali, mkulu wa…
Read More » -
Chichewa
Dzombe kukoma, koma…
Kuyambira makedzana, panthawi ya ulendo wa ana Aisiraele kuchoka ku Aigupto kupita kudziko lolonjezedwa lija la Kenani ngakhalenso nthawi…
Read More » -
Business News
Smiles amid frowns: the case of contract tobacco farmers
Listening to their stories one would think there is an invisible hand at play, and that words have been…
Read More » -
Nkhani
‘Luso la mpira ndilo lidandidolola’
Sabata zitatu zapitazo Sindi Simtowe adamanga ukwati ndi Ardron Msowoya, mnyamata yemwe akugwira ntchito ku Inde Bank. Kwa iwo amene…
Read More » -
Nkhani
Ulova wafika posauzana
Adatenga digiri ya uphunzitsi mu 2010 ku Chancellor College (Chanco), kaamba kosowa ntchito, tsopano wachoka m’tauni ndipo akukhala kumudzi komwe…
Read More » -
National Sports
Balaka Stadium turns into battlefield again
Questions on whether Balaka Stadium is fit to host big matches arose again on Saturday when a quarter-final match…
Read More » -
Chichewa
Richard Mbulu: Chilombo cha Mafco FC
Dzina la Richard Mbulu lasanduka nyimbo ya mizinda yonse chifukwa cha ntchito zake zomwetsa zigoli. Pano Mbulu akutsogola mu…
Read More » -
Chichewa
Avulaza shehe akuitanira mapemphero
Nthawi ikamathamangira 5 koloko mmawa, anthu achipembedzo cha Chisilamu amadzutsidwa kuti akachite mapemphero kumzikiti pamene shehe kapena mwazini (muezzin)…
Read More » -
Chichewa
Lonjezo la jb Lasanduka loto
Bambo ake adamwalira, chiyembekezo chidali pa bambo womupeza, nawonso adamukhumudwitsa pomugwiririra n’kumupatsa pathupi ndipo bwalo la milandu lidamugamula kuti…
Read More » -
Chichewa
Alimi samalani pososa
Mlimi weniweni ndiye amasamalitsa kalendala yake ya ulimi. Kuyambira mwezi watha mpaka uno, alimi amalangizidwa kuti akuyenera kuyamba kusosa. Mlangizi…
Read More » -
Front Page
Mbulu on sa Club radar
TNM Super League current top goal scorer Mafco striker Richard Mbulu’s exploits have attracted the interest of South Africa’s Premier…
Read More » -
Nkhani
‘Akudyerera obwela’
A malawi akhala akuingidwa ngati nkhuku m’maiko ena akafuna thandizo la chipatala, koma nzika zakunja kumadzawamwera mazira zikafika m’dziko muno…
Read More » -
Nkhani
Alipa nkhuku 70 atatayira chimbudzi pachitsime
Gulupu Chinyamula kwa T/A Kamenyagwaza m’boma la Dedza walipitsa amayi awiri nkhuku 35 aliyense chifukwa chotaira chimbudzi pachitsime. Iye walamulanso…
Read More »