-
Nkhani
‘Idali nthawi ya mapemphero’
Mtsikana akadzakulembera SMS yoti ‘I care for you’ ndiye kuti zatheka chifukwa uthengawu ndi waukulu kwambiri. Zidayambanso choncho ndi Alison…
Read More » -
Chichewa
MOYO UKUTHINA
Amalawi ena ati mavuto ankitsa ndipo akusowa mtengo wogwira pamene akadaulo a zachuma akuti mavutowa afikanso pena chifukwa cha…
Read More » -
Chichewa
Maule akusambabe wamkaka
Khomo la ukwati silisowa. M’banja la Nyasa Big Bullets kudakali chisangalalo kutsatira chipambano chawo pobabata asilikali a ku Mzuzu,…
Read More » -
Chichewa
Taphulanji m’zaka 52?
Anthu komanso atsogoleri ena ati zaka 52 za ufulu wodzilamulira zomwe dziko la Malawi lidakwanitsa Lachitatu ndi nthabwala chabe…
Read More » -
Chichewa
Kodi Chipuwa wabwerera kumalonda?
Luso la Richard Chipuwa, goloboyi wa Flames komanso Mighty Be Forward Wanderers ndi losayamba. Pa 15 January chaka chino…
Read More » -
Nkhani
Ati boma lisabweze ndalama ku FDH
Anthu ena otsata mmene zinthu zikuyendera m’dziko muno aopseza kuti akonza zionetsero ngati boma limvere zonena za banki ya FDH…
Read More » -
Nkhani
Okwiya aimitsa kumanga njanje
Madzi achita katondo ku Nkaya m’boma la Balaka komwe anthu okwiya aletsa kampani ya Mota Engil yomwe ikumanga njanje kumeneko…
Read More » -
Chichewa
Othawa nkhondo akutuwa ndi njala
Kwathina kukampu ya anthu othawa nkhondo m’dziko la Mozambique amene akukhala ku Mwanza ndi Neno komwe anthuwa akutuwa ndi…
Read More » -
Chichewa
‘Mudali m’galimoto ulendo ku Area 23’
Kumwetulira kwa Shreen Mbendera, muulutsi pawailesi ya Galaxy FM, kunachititsa kuti Kimu Kamau amuthere mawu namwaliyu. Ukwati walengezedwa kale…
Read More » -
Chichewa
Zikhulupiriro zina Zisokoneza mdulidwe
Zikhulupiriro zosiyanasiyana zikusokoneza ntchito ya mdulidwe wa abambo womwe unduna wa zaumoyo komanso mabungwe akulimbikitsa, Msangulutso wapeza. Ku Nsanje,…
Read More » -
Chichewa
Mike Mkwate: Chilombo pakati pa Bullets
Dzina la Mike Mkwate si lachilendonso m’dziko muno malinga ndi ntchito yomwe akuphika ku Nyasa Big Bullets. Wasewera magemu…
Read More » -
Nkhani
Boma libweza moto pa zolipiritsa m’zipatala
Ganizo la boma loyambitsa mbali yolipiritsa m’zipatala zonse za boma kuyambira July akubwerayu, lalephereka, nduna ya zaumoyo, Peter Kumpalume, yatero.…
Read More » -
Nkhani
Asing’anga akuti akonza zionetsero
Asing’anga m’dziko muno akonza zionetsero zokhumudwa ndi chigamulo cha bwalo lalikulu la Mzuzu chopereka chiletso kuti asiye kugwira ntchito yawo…
Read More » -
Business News
Exposing the power of cooperatives
For a long time, they have been operating their business and producing goods without certification from Malawi Bureau of…
Read More » -
Chichewa
Mnyamata asiya sukulu chifukwa cha mantha
A makhumbira atakhala msirikali, koma popanda moyo ntchitoyi singatheke. Lero Christopher Robert, mnyamata wachialubino, wasankha kaye moyo posiya sukulu…
Read More » -
Chichewa
Asing’anga asowa mtengo wogwira
Chigamulo cha bwalo lalikulu ku Mzuzu kuletsa asing’anga kuti asagwirenso ntchito m’dziko muno zabweretsa mpungwepungwe ndipo asing’anga eniake akuti…
Read More » -
Chichewa
‘Lidali tsiku la Big Sunday’
Sangwani Mwafulirwa tsopano ndi bambo, si mnyamatanso monga ena akumudziwira chifukwa dzulo pa 4 June 2016 wamulonjeza Trufena Chiwaya,…
Read More » -
Chichewa
Pezani umuna wa ng’ombe
Nthawi yokhala ndi ng’ombe za makolo yapita. Ndi K1 500 yokha, alimi akhoza kupeza umuna wa ng’ombe za makono.…
Read More » -
Chichewa
‘Akwawo ankati Ichocho ndi choopsa’
Ntchito ndi maonekedwe a Yasin ‘Ichocho’ Suwedi, mmodzi mwa akatswiri pankhani yofufumitsa minyewa, ndizo zidali zolepheretsa kuti akwatire Fatima…
Read More » -
Chichewa
Obindikira m’nyumba azengedwa mlandu
Bwalo la milandu la majisitireti mumzinda wa Blantyre lakhazikitsa Lachitatu, 25 May, ngati tsiku lomwe lidzapereke chigamulo kwa banja…
Read More »