-
Nkhani
Ulendo womaliza wa Grace Chinga
Thupi la Grace Chinga yemwe adamwalira Lachitatu usiku liikidwa lero m’manda a HHI mumzinda wa Blantyre. Thupi la Grace limayembekezeka…
Read More » -
Chichewa
Kodi Idrissa Walesi akutani mu Mozambique?
Mu 2012 ku Mighty Wanderers kudatchuka wosewera wa kumbuyo, Idrissa ‘baba’ Walesi. Atangotchuka, Walesi adasowa ndipo zidamveka kuti wakwawira…
Read More » -
Chichewa
Dovu lakula ku nsanje
Anthu ena m’boma la Nsanje alephera kupirira nkhuli ndipo akuphabe ndi kugulitsa nyama ya ng’ombe, mbuzi, nkhumba ndi nkhosa…
Read More » -
Chichewa
‘Kudali ku Presbyterian Church of Malawi’
Kudali kuphwanya mafupa ku Dream Centre Assemblies of God mumzinda wa Blantyre Loweruka pa 2 May pamene Faith Mussa amachititsa…
Read More » -
Nkhani
‘Palibe angamange mvula, siyani kuzunza anthu’
Masiku apitawa anthu 7 adawagwira ku Chiradzulu ndipo adawazunza powaganizira kuti akumanga mvula. Adawakolezera moto masanasana kuti aothe ndipo akuti…
Read More » -
‘Omanga mvula’ awaothetsa moto likuswa mtengo’
Kudali gwiragwira Loweruka lapitalo m’midzi ya Kazembe, Golosi ndi Ntamba kwa T/A Nkalo m’boma la Chiradzulu pamene anthu olusa…
Read More » -
Business News
Grow sorghum to counter climate change—Minister
Minister of Agriculture, Irrigation and Water Development Allan Chiyembekeza has urged farmers to consider diversification by growing sorghum to…
Read More » -
Chichewa
Wonyozedwa ali moyo Alemekezedwa atamwalira
Gogo wina ku Ntcheu, yemwe amagona pachisakasa chonga pogulitsira tomato abale ake akukana kuti agone m’nyumba yabwino, adalemekezedwa atamwalira…
Read More » -
National Sports
Mpulula happy with new players at Max Bullets
Max Bullets coach Leo Mpulula is a happy man now with the arrival of new experienced players who have…
Read More » -
Nkhani
Chimanga chikololedwa chochepa—Unduna
Kauniuni woyamba wa zokolola wasonyeza kuti chaka chino Amalawi akolola chimanga chocheperako kusiyana ndi chaka chatha, chikalata chimene unduna wa…
Read More » -
Nkhani
‘Apolisi adalakwa pomanga aphungu’
Katswiri wina wa za malamulo ndi anthu ena othirapo ndemanga agwirizana ndi bungwe la Malawi Law Society (MLS) ponena kuti…
Read More » -
Chichewa
‘Mudali mu Sitandede 1’
Dzina la Julius Mithi si lachilendo. Ndi kadaulo pa zowerengetsa komanso wagwirapo ntchito kubungwe la zamasewero la FAM. Ngakhale…
Read More » -
Editors Pick
Man shot, arrested for Bingu Stadium vandalism
Police in Lilongwe on Monday night shot and arrested a 30-year-old-man for allegedly attempting to steal pipes at Bingu National…
Read More » -
Front Page
Politicians scramble to attend PAC meet
There is confusion among political parties towards the Public Affairs Committee (PAC) Fifth All-inclusive Stakeholders’ Conference as in a last-minute…
Read More » -
Chichewa
Ndaziona: Aona kuwala ku Mozambiki
Mwezi wathawu osewera awiri, Ndaziona Chatsalira ndi Green Harawa adachoka ku Silver Strikers ulendo ku Mozambique kukasaka moyo wina. Chatsalira…
Read More » -
Chichewa
Zikavuta, nawo anthu amakoka ngolo
Ngolo imakokedwa ndi ng’ombe kapena abulu, koma pena zikavuta nawo anthu amakoka. Pachithunzipa, anyamatawa adakoka ngoloyi ng’ombe zitathawa. Nanga titani?…
Read More » -
Chichewa
Amukwenya ponena olumala kuti ‘agalu’
Banja lina lapempha mkulu woyang’anira za maphunziro m’maboma a Phalombe, Mulanje ndi Thyolo (Divisional Education Manager—DEM) kuti athane ndi…
Read More » -
Nkhani
Miyezi ikutha osalandirandalama za mthandizi
Akugona ndi njala, ena akudya nyanya (mizu ya mitengo yoyanga) pamene akudikirirabe ndalama zawo za ntchito ya mthandizi yomwe…
Read More » -
National News
Press Trust plants trees in Nsanje
As one way of mitigating climate change in Nsanje, Press Trust on Tuesday led communities in the district to…
Read More » -
Nkhani
Apolisi akwidzinga anthu 10 ku Neno
Akuwaganizira kuti adatengapo mbali kupha agogo anayi Apolisi m’boma la Neno Lachinayi adanjata anthu 10 powaganizira kuti adatengapo mbali pa…
Read More »