-
Nkhani
Kutambasula nthenda ya kadzamkodzo
Kunjaku kuli nthenda zosiyanasiyana koma nthenda zina ukamva, kudulitsa mutu wazizwa. Sabata yapitayi, nduna ya zaumoyo, Dr Peter Kumpalume, adatsogolera…
Read More » -
Chichewa
Tidziwane ndi Enock Balakasi wa Joy Radio
Atolankhani m’dziko muno amakumana ndi zokhoma zambiri makamaka pofuna zoti auze mtundu wa Amalawi. Mwa zifukwa zina, kusoweka kwa lamulo…
Read More » -
Nkhani
Katundu wobwera ku Malawi ali pachiopsezo ku Mozambique
Magulu a zachifwamba m’dziko la Mozambique akuchitira mtopola galimoto zonyamula katundu wosiyanasiyana wobwera m’dziko muno kuchokera kumaiko ena podutsa m’dzikolo.…
Read More » -
Nkhani
Olowa m’dziko mozemba aonjeza mavuto m’ndende
Mavuto a m’ndende za m’dziko muno ngosakamba koma kafukufuku wa Tamvani wasonyeza kuti ena mwa mavutowa akudza kaamba ka anthu…
Read More » -
National News
Kachere Reformatory gets shot in the arm
Kachere Prison in Lilongwe, a reformatory centre for young offenders, on Sunday received a kitchen facility and other materials…
Read More » -
Chichewa
‘Kudali kukwaya ku Mtima Woyera’
Udali ulendo wokhetsa thukuta lowopsa kuti zonse zilongosoke pakati pa Gray Lizimba ndi Iness Chimombo koma zonse zidafika pampondachimera…
Read More » -
Chichewa
Milandu ya maalubino Izipita kukhothi lalikulu
Milandu yokhudza kuphedwa kapena kusowetsedwa kwa maalubino tsopano akuti izikakambidwira mukhothi lalikulu lomwe lili ndi mphamvu yopereka chilango chokhwimirapo…
Read More » -
Chichewa
Blessings Cheleuka wa pa JOY FM
Amalawi ambiri kuyamba Lolemba mpaka Lachisanu nthawi ya 2 koloko kufika 4 koloko masana amatsegula wailesi ya Joy FM kuti…
Read More » -
Chichewa
‘Timakakonza za ntchito’
Wakaona nyanja adakaona ndi mvuwu zomwe. Mauwa apherezedwa ndi ukwati wa Amos Mazinga wa ku Dowa m’mudzi mwa Ngozi,…
Read More » -
Chichewa
Henry Mussa: Akusowa tulo ndi Teba
Anthu omwe adagwirako ntchito m’migodi ya m’dziko la South Afrika pamgwirizano wa Temporary Employment Bureau of Africa (Teba) kapena…
Read More » -
Chichewa
Mafupa a alubino si chizimba—sing’anga
Mwadzidzidzi, dziko la Malawi latchuka ndi mbiri yomvetsa chisoni komanso yochititsa manyazi. Iyitu ndi nkhani yozembetsa ndi kupha maalubino ati…
Read More » -
National News
Albinos, CSOs petition police
People with albinism joined by civil society organisations (CSOs) yesterday marched to Police headquarters in Lilongwe to present a…
Read More » -
National News
Chiluzi upgraded to full primary school
Chiluzi Primary School in Traditional Authority (T/A) Kasumbu in Dedza is now a full primary (FP) courtesy of Nora…
Read More » -
Chichewa
Phyzix wadza ndi Captain Long John
Patapita zaka zingapo akutchuka ndi nyimbo zomwe zidavuta monga Cholapitsa, Gamba, Chilombo, Abwana, Memba, Town Monger, Man phyzo, Handsome,…
Read More » -
Chichewa
Amalawi valani dzilimbe—Mutharika
Mtsogoleri wa dziko lino Peter Mutharika dzulo watsegulira nkhumano ya aphungu a Nyumba ya Malamulo yokambirana ndondomeko ya…
Read More » -
Nkhani
Akati ‘tonde azimveka fungo’ akutanthauzanji?
Miyambi ilipo yosiyanasiyana ndipo ina ukaimva mutu umachita kuwira, kulephera kulumikiza mwambiwo ndi tanthauzo lake. Ena amangoti bola ndanenapo mwambi…
Read More » -
Nkhani
Kusowa kwa madzi kusokoneza zambiri ku Lilongwe
Chidziwitso cha Lilongwe Water Board (LWB), bungwe lopopa ndi kugawa madzi mumzinda wa Lilongwe, choti madzi akhala akuvuta kufikira dzinja…
Read More » -
Chichewa
Chipatala chiutsa mapiri pachigwa
Akuluakulu ena a khonsolo ya Lilongwe ndi kontilakitala yemwe akumamanga chipatala cha Biwi mumzinda wa Lilongwe, ayankha mafunso zitadziwika…
Read More » -
Chichewa
‘Adali kasitomala wa mchemwali wanga’
Mchemwali asamangokhala wokuphikira nsima kapena kukuthandiza kuchapa zikavuta, nthawi zina azikhalaso njira yokulondolera njira ya komwe kuli mbali ya…
Read More » -
Chichewa
Wa ku Mangalande anjatidwa atagwiririra wa ku Amerika
Bwalo la Chief Resident Magistrate ku Lilongwe lagamula nzika ya dziko la ku Britain Amrish Magecha kukaseweza zaka 8…
Read More »