-
Nkhani
A Mpesi atula pansi udindo
Pomwe kwatsala masiku 30 enieni kuchoka lero kuti chisankho chapadera m’madera angapo chidzachitike, mkulu woyendetsa zisankho ku bungwe la Malawi…
Read More » -
National News
Rift Valley Fever disease hits Southern Region—ministry
Ministry of Agriculture, Irrigation and Water Development has confirmed a Rift Valley Fever (RVF) outbreak in Chiradzulu District and surrounding…
Read More » -
Nkhani
When mob justice myths leave trail of blood
Like any other day, dawn broke peacefully on Saturday, May 9, as 42-year-old Madalitso Joe William went about his daily…
Read More » -
Nkhani
Kafukufuku wa ndege wayamba
Amalawi tsopano maso ali gaaa pa komiti yapadera ya ku Nyumba ya Malamulo yomwe ikufufuzanso chomwe chidachititsa ngozi ya ndege…
Read More » -
Nkhani
Kulibe kuzondana kaamba ka kusowa kwa mafuta
Amalawi tsopano ayamba kulingalira mozama asadapange ulendo kuopa kuti angakwangule konse kamthumba komwe khomo likuyang’anira pa zosowa zonse kaamba ka…
Read More » -
Nkhani
Chikho cha fodya chasefuka
Chikho cha fodya chaka chino chasefukira ndi makilogalamu 27 miliyoni zomwe zabweretsa nkhawa yoti mtengo wake ukhoza kukhala wonyotsolera ku…
Read More » -
Nkhani
Amalawi akufinyika
Pamene mtengo wa mafuta udakwera Lachitatu sabata ikuthayi, Amalawi ochokera m’madera osiyanasiyana m’dziko lino ati kulira n’kosayamba. Koma ikakuona litsiro…
Read More » -
Nkhani
Kampeni itha mawa
Pomwe Chisankho Chapadera chikuchitika m’madera a aphungu 4 ndi makhansala 9 Lachiwiri, kampeni yovomerezeka imene idayamba pa 15 January itha…
Read More » -
Nkhani
Alangiza MEC isake njira yobweretsera mabaloti
Mkulu wa bungwe lolimbikitsa demokalase la Centre for Multiparty Democracy (CMD) a Boniface Chibwana aunikira bungwe la Malawi Electoral Commission…
Read More » -
Nkhani
Otsutsa aopseza kunyanyala zokambirana atamangidwa
Aphungu otsutsa boma ku Nyumba ya Malamulo aopseza kuti zomanga aphungu mwachisawawa zikapitirira iwo a zinyanyala ntchito za ku nyumbayo…
Read More »