-
Nkhani
Mkokemkoke pa za maufumu
Pali mkokemkoke pakati pa maufumu a m’dziko lino ndi boma pa malire amene mbali ziwirizi zingatenge potsatira malamulo. Chikalata chimene…
Read More » -
Nkhani
‘Lamya zikadathandiza kafukufuku wa ndege’
Lamya za m’manja za omwe adali m’ndege ya asilikali a nkhondo yomwe idagwera ku Chikangawa zikadapezeka msanga n’kuchitidwa chipikisheni zidakatha…
Read More » -
Nkhani
Achenjeza maboma 23 za nyengo ya el nino
Nthambi yoona za ngozi zogwa mwadzidzidzi ya DoDMA yachenjeza kuti ulosi woyamba wa nyengo ya mvula ya chaka chino wasonyeza…
Read More » -
Nkhani
Alangiza aphungu achepetse tulo
Aphungu a ku Nyumba ya Malamulo adakwangula mkumano wawo sabata yatha atadutsitsa mabilu 14 omwe ambiri akukhudza za chuma ndi…
Read More » -
Nkhani
Aphungu ayembekezere mtsutso wokhetsa thukuta
Pomwe mkumano wa aphungu udayamba Lachiwiri pa 7 July, 2026, nkhani mkati mwa sabatayi zasonyeza kuti mbali yomwe siidakonzekere bwino…
Read More » -
Front Page
Panic as millions get netted out of social protection
Malawi’s social protection efforts are in disarray as donors flee and budget allocations collapse, leaving the sector’s specialists gathering in…
Read More » -
Nkhani
A Mpesi atula pansi udindo
Pomwe kwatsala masiku 30 enieni kuchoka lero kuti chisankho chapadera m’madera angapo chidzachitike, mkulu woyendetsa zisankho ku bungwe la Malawi…
Read More » -
National News
Rift Valley Fever disease hits Southern Region—ministry
Ministry of Agriculture, Irrigation and Water Development has confirmed a Rift Valley Fever (RVF) outbreak in Chiradzulu District and surrounding…
Read More » -
Nkhani
When mob justice myths leave trail of blood
Like any other day, dawn broke peacefully on Saturday, May 9, as 42-year-old Madalitso Joe William went about his daily…
Read More » -
Nkhani
Kafukufuku wa ndege wayamba
Amalawi tsopano maso ali gaaa pa komiti yapadera ya ku Nyumba ya Malamulo yomwe ikufufuzanso chomwe chidachititsa ngozi ya ndege…
Read More »