Nkhani
-
Akuti zipolowe zichepe
Zipolowe kaamba ka ndale zomwe zakhala zikuchitika m’dziko muno zikupereka chiopsezo kuchisankho cha chaka chamawa komanso kutekesa mtendere wa dziko…
Read More » -
‘JB watukula amayi, koma ntchito ikadali’
Pamene dziko la Malawi lagwirana manja ndi maiko ena padziko lapansi pokukumbukira tsiku la amayi, Amalawi ena athirapo ndemanga ndi…
Read More » -
Zipolowe atamangidwa Mutharika
Kumangidwa kwa anthu 11 omwe akukhudzidwa ndi nkhani yofuna kulanda boma Bingu wa Mutharika atamwalira sikudakomere anthu ena amene adachita…
Read More » -
Lipoti la imfa ya Bingu latekesa boma, DPP
Pomwe Malawi waona utsi wokhetsa misozi chifukwa cha kumangidwa kwa mamulumuzana a DPP komanso amaudindo ena m’boma, akadaulo pazandale komanso…
Read More » -
Ndalama zakale zitha pa 23 May
Banki yaikulu yakumbutsa mabanki a m’dziko muno kuti ndalama zakale za ‘Chilembwe’ dziko lino zisiya kugwira ntchito pa 22 May.…
Read More » -
‘Chibaluwa chasiya zina’
Pamene kwangotha sabata mpingo wa katolika utatulutsa chikalata chounikira momwe zinthu zikuyendera m’dziko muno, katswiri wa ndale kusukulu ya ukachenjede…
Read More » -
Akulimbana ndi Edzi
Pothandiza kuti uthenga wokhudza matenda a EDZI ufikire achinyamata ambiri makamaka pobweretsa uthengawo pafupi ndiponso kunjira zomwe achinyamata akugwiritsa ntchito…
Read More » -
Gawo 65 lavuta
DPP inenetsa sipikala achotse aphungu ochoka chipani Chipani cha DPP chati sichilola kuti nkhani yokhudza Sekishoni 65 yomwe imapatsa mphamvu…
Read More » -
Sitalaka yatha, yaika amalawi pamoto
Pomwe ogwira ntchito m’boma ali pa sitalaka kufuna kuti malipiro awo akwere ndi K67 pa K100 iliyonse, anthu omwe amafuna…
Read More » -
‘Mawu a JB ndi loto’
Akuluakulu a mabungwe ena ati mawu a mtsogoleri wa dziko lino Joyce Banda potsegulira msonkhano wa aphungu Lachisanu lapitalo ndi…
Read More »