Chichewa
-
‘Chuma chifike kumudzi’
Nduna ya za chuma a Joseph Mwanamvekha ati ndondomeko ya za chuma imene apereka m’Nyumba ya Malamulo dzulo ikuonetsetsa kuti…
Read More » -
Samalani ndi nyongolosi nthawi ya mvula ino
Kale alimi a m’gulu la ulimi wa ng’ombe la Chilangoma kwa mfumu yaikulu Kuntaja m’boma la Blantyre samapindula ndi ulimiwu…
Read More » -
Apereka katemera wachigodola kwa ng’ombe
Khonsolo ya boma la Nsanje kudzera ku nthambi yoona za ulimi wa ziweto yati yapereka katemera wachigodola, Foot and Mouth…
Read More » -
Otsutsa aopseza kunyanyala zokambirana atamangidwa
Aphungu otsutsa boma ku Nyumba ya Malamulo aopseza kuti zomanga aphungu mwachisawawa zikapitirira iwo a zinyanyala ntchito za ku nyumbayo…
Read More » -
Low turnout as voter registrationfor March 17 by‑elections opens
Voter registration for the March 17 by‑elections opened on a muted note with several registration centres recording little or no…
Read More » -
Adagona ndi mwana, kapena ayi?
Zodulitsa mutu wa zizwa. Pomwe bwalo la milandu la majisitileti ku Mchinji lidagamula kuti a Ernest Chimpeni a zaka 37…
Read More » -
Chimanga ‘amachibisa’ chatuluka
Patangotha masiku ochepa boma litayamba kulandira chimanga chomwe lagula m’dziko la Zambia, mavenda nawo atulutsa chimanga chawo chomwe akufuna kukagulitsa…
Read More » -
Kulembetsa ndi lero
Kalembera wa Chisankho Chapadera cha pa 17 March chikubwerachi ayamba lero m’madera a aphungu 4 ndi makhansala 9 m’maboma 12…
Read More » -
Samalani, kunjaku kwabuka cholera
Boma lalandira matamando pa momwe layendetsera dziko m’masiku 100 oyambirira koma malesawa akumana n’chipsinjo cha matenda a cholera omwe abuka…
Read More » -
Zaka zisanu chifukwa choba katundu
Bwalo la First Grade Magistrate ku Lilongwe, Lachinayi lidagamula Mayi Esther James a zaka 38 kuti akakhale ku ndende kwa…
Read More »