Chichewa
-
Mlangizi wa Peter wati akaone zina
Ben Phiri, mlangizi komanso wothandizira Pulezidenti Peter Mutharika, Lachiwiri adati watula pansi udindo wake pofuna kupereka mpata woti amufufuze…
Read More » -
Bajeti isautsa Amalawi
Patenga nthawi kuti Amalawi adzamwetulire kutsatira ndondomeko ya zachuma yomwe nduna ya zachuma Goodall Gondwe adapereka ku Nyumba ya…
Read More » -
Kachiza back to amateur boxing
After suffering a second-round knockout defeat to Zimbabwean boxer Tinashe Mwadziwana during their 12-round non-title professional bout in Lilongwe, two…
Read More » -
Tadeyo Mliyenda: Polisi Palibe yalowa bwemba
Tsiku limenelo pa Wenela padavuta zedi. Padafika sing’anga wina adali ndi mitu inayi. Masalamusiwo adachitika dzuwa likuswa mtengo. Chomwe chidandichititsa…
Read More » -
Tame Mwawa: Chiphwanya wa Tikuferanji
Sewero la Tikuferanji ndi limodzi mwa masewero omwe amapereka phunziro kwa anthu pazochitika mmoyo wa tsiku ndi tsiku komanso ndi…
Read More » -
Akufuna mwana
Akufuna mwana Zikomo Gogo Banja ndi mwamuna wanga lidatha mu 2011. Ndidapeza mwamuna wina yemwe timamvana ndipo tidakayezetsa komwe adatipeza…
Read More » -
Tracing economic growth drivers
In 2012, a slump in agriculture resulting from a weather-related decline in maize production and a halving of the…
Read More » -
Sangie to perform in Jamaica
Fortune has landed on Malawi’s rising dancehall artist Angel Mbekeani, better known by her stage name Sangie, having being…
Read More » -
Anatcheleza: Akundiopseza a gogo wanga
Akundiopseza Gogo wanga, Ndili ndi zaka 24 ndipo ndimachokera kwa Kachere mumzinda wa Blantyre koma pano ndili ku Mangochi kumene…
Read More » -
Tadeyo Mliyenda: Ulendo wa ku Mzuzu
Tsikulo Abiti Patuma adandipeza pa Wenela kuti ndimuperekeze ku Mzuzu kumene amakacheza ndi Paparazzi komanso anzake. Tidakwera basi yausiku pa…
Read More » -
Bwalo La Ulimi: Ma trawler aunikidwe
Trawler ndi sitima kapena boti lokhala ndi injini yapakati mphamvu ndithu imene imakoka ukonde wa maso osachepera mamilimita 38 ndipo…
Read More » -
Tomato wabooka pa Bembeke
Alimi ku Bembeke m’boma la Dedza ayamba kufupa tomato wawo pamene wachoka pa mtengo wa K6 000 pa dengu kufika…
Read More » -
Ulangizi wa pafoni uthandiza alimi
Ndizachidziwikile kuti dziko la Malawi limadalira ulimi pa chuma chake ndipo ambiri mwa alimi m’dziko muno ndi alimi a minda…
Read More » -
Muli phindu mu ulimi wa chinangwa
Mlimi amaonetsa chitsakano ngati akupindula ndi mbewu zake. Ulimi weniweni umakhala umenewu woti mlimi azipindula kusiyana nkuti azikhalira kukanda m’mutu…
Read More » -
Alimi samalani thonje, kwagwa kachilombo koononga
Kwatulukira kachilombo kotchedwa kodikodi kapena kuti mealybug kamene kakuononga thonje, watero mlembi wamkulu wa unduna wa malimidwe Erica Maganga. Maganga…
Read More » -
Local entrepreneurs lack patriotism
TRINTAS MANDA* One does not need to be a university graduate to appreciate the socio-economic impact the resurgence of xenophobia…
Read More » -
‘Community colleges to spur job creation’
Government is optimistic that the establishment of community colleges will spur opportunities for jobs among youths and eventually stimulate the…
Read More » -
Caled donates writing materials to Ntchisi pupils
Centre for Agricultural Labour Efficiency and Development (Caled) on Tuesday donated notebooks, pens and pencils to 292 pupils and boxes…
Read More » -
Tadeyo Mliyenda: Malingaliro padziko
Ndidakhala pa Wenela kudya mpweya. Minibasi zoti ndiyitanire abale anzanga, osabwera n’komwe. Ndidagwera m’maganizo. Ndidakumbukira zoti pali mkulu wina yemwe…
Read More » -
Big Interview: Georgina Phiri, kids party organiser
Her passion for children led her to open up a business of organizing themed parties for them. The world of…
Read More »