Chichewa
-
Ndikulemba anthu 200—a Mutharika
Mtsogoleri wa dziko lino a Peter Mutharika adzudzula anthu omwe akuti amawanena m’masamba a mchezo kuti sadalingalire amayi posankha maudindo…
Read More » -
Amalawi alankhula pa malonjezo
Amalawi ena ati mpofunika ndondomeko zogwirika kuti boma lomwe lalowa kumene la DPP likwaniritse malonjezo ake a m’manifesto. Ena mwa…
Read More » -
Chitonzo chakula
Mmodzi mwa akadaulo a momwe ziwalo za m’thupi zimagwirira ntchito, physiology, wati chiwerengero cha abambo amene amakayezetsa ngati ali obereka…
Read More » -
TIDAKUMANA: ‘Mudali mu Barbershop’
Lidali tsiku Lachisanu masana m’chaka cha 2012 ku Area 25 C ku Lilongwe ndipo kunja kudali kwa dzuwa pomwe Shingrai…
Read More » -
Apempha achinyamata asunge bata
Pamene dziko lino likukonzekera kuponya mavoti Lachiwiri likudzali, wapampando wa bungwe la Machinga District Youth Network a Mphatso Chikaonda apempha…
Read More » -
Lorani mtendere ulamulire
Kampeni ikutha mawa. Atsogoleri atambasula mfundo zawo za chitukuko zomwe zili m’manifesto. Nawo mabungwe a Oxfam ndi Women Legal Resource…
Read More » -
Mabungwe akufuna malamulo okhudza AI
Mabungwe a Centre for Human Rights and Rehabilitation (CHRR) ndi Malawi Human Rights Commission (MHRC) apempha boma kuti liunikenso malamulo…
Read More » -
Zikhalidwe zikukhomerera amayi
Wapampando wa Engalaweni Women Group a Mervis Mvula akuti zikhalidwe, zikhulupiriro ndi umphawi ndizo zikulepheretsa amayi ambiri kulowa ndale. A…
Read More » -
Dolo ndi ndani mu chipeta ichi?
Pamene kwatsala masiku atatu okha kuti nzika za dziko lino zivote, atsogoleri omwe akuimira pa mipando ya upulezidenti, uphungu wa…
Read More » -
Akufuna msewu, Admarc ku Tsangano However, the judge found that Chisale’s case did not meet the threshold for certification.
Mfumu yaikulu Mpando ku Ntcheu yalangiza boma kuti liganizire zomanga msika wokhazikika komanso msewu wabwino ku Tsangano m’boma la Ntcheu…
Read More »