Chichewa
-
Apempha achinyamata asunge bata
Pamene dziko lino likukonzekera kuponya mavoti Lachiwiri likudzali, wapampando wa bungwe la Machinga District Youth Network a Mphatso Chikaonda apempha…
Read More » -
Lorani mtendere ulamulire
Kampeni ikutha mawa. Atsogoleri atambasula mfundo zawo za chitukuko zomwe zili m’manifesto. Nawo mabungwe a Oxfam ndi Women Legal Resource…
Read More » -
Mabungwe akufuna malamulo okhudza AI
Mabungwe a Centre for Human Rights and Rehabilitation (CHRR) ndi Malawi Human Rights Commission (MHRC) apempha boma kuti liunikenso malamulo…
Read More » -
Zikhalidwe zikukhomerera amayi
Wapampando wa Engalaweni Women Group a Mervis Mvula akuti zikhalidwe, zikhulupiriro ndi umphawi ndizo zikulepheretsa amayi ambiri kulowa ndale. A…
Read More » -
Dolo ndi ndani mu chipeta ichi?
Pamene kwatsala masiku atatu okha kuti nzika za dziko lino zivote, atsogoleri omwe akuimira pa mipando ya upulezidenti, uphungu wa…
Read More » -
Akufuna msewu, Admarc ku Tsangano However, the judge found that Chisale’s case did not meet the threshold for certification.
Mfumu yaikulu Mpando ku Ntcheu yalangiza boma kuti liganizire zomanga msika wokhazikika komanso msewu wabwino ku Tsangano m’boma la Ntcheu…
Read More » -
Kandideti walonjeza nsapato, maendedwe otsika mtengo
Malonjezo pa nthawi ya chisankho si achilendo. Koma pali ena oti ukamva, umagwedeza mutu. Yemwe adzaimire chipani cha UTM ku…
Read More » -
Kandideti wa MCP wapambana anthu asanavote
Bungwe la zachisankho la Malawi Electoral Commission (MEC) lati yemwe amaimira chipani cha Malawi Congress Party (MCP) ku dera la…
Read More » -
Aphungu asintha lamulo
Fumbi lakhazikika lokhudza komwe anthu omwe adzakhale akugwira ntchito za chisankho pa nthawi yovota pa September 16 adzaponyere voti yawo.…
Read More » -
MEC yasefa ma kandideti, 17 adutsa
Pomwe kampeni ili mkati, bungwe la Malawi Electoral Commission (MEC) latulutsa maina a ma kandideti omwe akwaniritsa zofunika pa mpando…
Read More »