Chichewa
-
Chakwera, Nankhumwa akhambitsana
Chilinganizo chomwe chidaikidwa pofuna kuti mtsogoleri wa dziko lino Lazarus Chakwera akayankhe mafunso m’Nyumba ya Malamulo chidasanduka mtsutso pakati pa…
Read More » -
Akwapula mphunzitsi wochita ‘chisembwere’
Maphunziro a ana a Sitandade 8, adasokonera Lolemba pasukulu ya pulaimale ya Kalira, yomwe ili m’mudzi mwa Kanyera ku Mtakataka…
Read More » -
Okalamba 46 aphedwa zaufiti
Anthu okalamba 36 adaphedwa pakati pa January ndi December 2019 pomwe ena 10 adaphedwa pakati pa January ndi September 2020…
Read More » -
Chakwera wakwera paphiri
Akadaulo osiyanasiyana ati Pulezidenti Lazarus Chakwera waonetsa chamuna popita ku Nyumba ya Malamulo kukayankha mafunso a aphungu pankhani zokhudza dziko…
Read More » -
Anatchereza
Akufuna mwana Gogo, Ndakhala m’banja ndi mwamuna wanga zaka zisanu, koma wopanda mwana. Mwamuna wanga amalimbitsa mtima kuti ndisadandaule popeza…
Read More » -
Kudali ku msonkhano wa mapemphero
Mbusa Willard Maluwa yemwe akutsogolera mpingo wa Fountain of Victory m’boma la Salima adakumana koyamba ndi mkazi wake Abgail Mkwate…
Read More » -
Alimi alirira Admarc
Lipoti la nthambi yochenjeza anthu za njala ya Famine and Early Warning Network (FewsNet) lati alimi a chimanga akupitirira kulira…
Read More » -
Zotsamwitsa pa kutseguliranso sukulu
Pomwe ana asukulu akuyembekezera kutsegulira sukulu, aphunzitsi akuti sadakonzeke zokaphunzitsa chifukwa boma silikuonetsa chidwi pa nkhawa zawo. Mlembi wa bungwe…
Read More » -
Agwiriridwa ali mtulo
Pali zina zikamachitika, sungamvetse kuti zakhala bwanji. Mtsikana wina wa zaka 18 yemwe ali pabanja wagwiriridwa ali mtulo kumalo owedzera…
Read More » -
‘Kudali ku Spar ya ku City Centre’
Beatrice Mushani adakayamba ntchito ku Spar ya ku City Centre mu mzinda wa Lilongwe pa 1 October, 2018. Ndipo udali…
Read More »