Chichewa
-
‘Chidodo pamilandu’
Mitima ya Amalawi yayamba kuwira ndi chidodo chomwe chikuchitika pa milandu ina yomwe akadaulo akuti ndi mlingo omwe Amalawiwo akugwiritsa…
Read More » -
Chakwera akumbukira masiku 100 a Tonse
Lolemba, mtsogoleri wa dziko lino Lazarus Chakwera adali ndi mwambo wokumbukira kuti watha masiku 100 akulamula dziko lino. Pamwambo umene…
Read More » -
‘Amalawi dekhani’
Mtsogoleri wa dziko lino Lazarus Chakwera wati Amalawi asayembekezere kuti zonse zomwe adalonjeza nthawi ya kampeni zingakwaniritsidwe nyengo yochepa chifukwa…
Read More » -
Aphunzitsi akhala ndi khonsolo
Unduna wa za maphunziro wati ukufuna kukhazikitsa khonsolo ya aphunzitsi yoti izikhazikitsa mwambo komanso kutukula ntchito yauphunzitsi. Nduna ya za…
Read More » -
Akumba manda m’khonde la nyumba
Athu okwiya aika maliro pakhomo pa mkulu wina ku Chirimba mumzinda wa Blantyre yemwe amamanga nyumba panjira yolunjika kuchipata cha…
Read More » -
Aphungu akana makondomu aulere
Aphungu a Nyumba ya Malamulo Lachitatu adabweza mphatso ya makondomu 206 000 yomwe bungwe la Aids Health Foundation (AHF) lidapereka…
Read More » -
Takana kupha makanda
Ife sitivomera kupha makanda.” Uwu ndi uthenga womwe aphungu a Nyumba ya Malamulo auza Tamvani kuti aombera bilo yopatsa mwayi…
Read More » -
182 adzipha mu sept
Chiwerengero cha anthu omwe akudzipha chikunka chikwera m’dziko muno. Kafukufuku amene Msangulutso adapanga akuonetsa kuti sipakutha sabata osamva nkhani kuti…
Read More » -
Akupha makwacha ndi kuchulukitsa mbuzi za chi ‘boer’
Mmalo mopeza K20 000 ku mbuzi yaikulu bwino yachikuda imene imatenga miyezi yosachepera 6 kuti ikule bwino, Allan Kalimasiya wa…
Read More » -
Thirani manyowa mwachangu
Woona za kafukufuku wa za nthaka ku nthambi ya zakafukufuku wa zaulimi ya Bvumbwe m’boma la Thyolo Peter Mfune akuti…
Read More »