Chichewa
-
Sandulizani tomato, iphani makwacha
Pamene m’nyengoyi tomato amatsika mtengo chifukwa cha kuchuluka pamsika, katswiri pa luso lopanga zakudya zosiyanasiyana kuchokera ku mbewu za zipatso…
Read More » -
Malingaliro pa malonjezo a Tonse
Boma lolamula la Tonse Alliance lidalonjeza zambiri panyengo ya kampeni. Padutsa miyezi iwiri tsopano kuchoka pomwe mgwirizanowo udalowa m’boma ndipo…
Read More » -
Abwekera tomato wa ufa
Tomato waufa amasungika kwa zaka ziwiri, mtengo wake ndi golide kale komanso ndiwo zake zimakhala za maonekedwe a pamwamba .…
Read More » -
Kwaterera ku DPP
Madzi achita katondo kuchipani cha Democratic Progressive Party (DPP) chomwe chidali m’boma kwa zaka 6 zapitazo ndipo chidagwetsedwa ndi m’gwirizano…
Read More » -
Anatchereza
Ndipite kwa asing’anga? Zikomo Anatchereza, Palitu mkazi amene amandizunguza bongo. Mtima wanga nthawi zonse umakhala pa iye ndipo sindigona tulo…
Read More » -
Njiru yafika pena
Bambo wina wa zaka 30, ali m’chitokosi cha apolisi pomuganizira kuti adapha mwana wake wa zaka 7, ku Chileka mumzinda…
Read More » -
Osangoti neba akuweta nkhumba
Atangomva kuti ulimi wa nkhumba ndi waphindu Leckner Kanyama wa m’boma la Lilongwe adayamba ulimiwu mwansangala poganiza kuti atola chikwama.…
Read More » -
zofunika kulingalira potsegulira sukulu
Miyezi 5 yatha tsopano ana asukulu ali pakhomo chifukwa cha mliri wa Covid-19. Iyi ndi nkhani yomwe yasautsa ndikuyimitsa mitu…
Read More » -
Malingaliro Potsegulira sukulu
Dziko la Malawi latekeseka ndi nkhani yotsegulira sukulu ndipo pofuna kuonetsetsa kuti miyoyo ndi yotetezedwa komanso ufulu wa ophunzira usapitirire…
Read More » -
Nkhumba zimalira chisaliro
Chimodzimodzi ulimi wina ulionse, ulimi wa nkhumba uli ndi ndondomeko yake yoyenera kutsatira poweta kuti mlimi apindule. Mphunzitsi wa zaulimi…
Read More »