Chichewa
-
‘Chibaluwa chasiya zina’
Pamene kwangotha sabata mpingo wa katolika utatulutsa chikalata chounikira momwe zinthu zikuyendera m’dziko muno, katswiri wa ndale kusukulu ya ukachenjede…
Read More » -
Akulimbana ndi Edzi
Pothandiza kuti uthenga wokhudza matenda a EDZI ufikire achinyamata ambiri makamaka pobweretsa uthengawo pafupi ndiponso kunjira zomwe achinyamata akugwiritsa ntchito…
Read More » -
Gawo 65 lavuta
DPP inenetsa sipikala achotse aphungu ochoka chipani Chipani cha DPP chati sichilola kuti nkhani yokhudza Sekishoni 65 yomwe imapatsa mphamvu…
Read More » -
Sitalaka yatha, yaika amalawi pamoto
Pomwe ogwira ntchito m’boma ali pa sitalaka kufuna kuti malipiro awo akwere ndi K67 pa K100 iliyonse, anthu omwe amafuna…
Read More » -
‘Mawu a JB ndi loto’
Akuluakulu a mabungwe ena ati mawu a mtsogoleri wa dziko lino Joyce Banda potsegulira msonkhano wa aphungu Lachisanu lapitalo ndi…
Read More » -
‘Ngakhale odulidwa kale adulidwe’
Amuna amene adadulidwa potsatira chipembedzo kapena chikhalidwe ayenera kudulidwanso, ngati sanadulidwe moyenera, watero mkulu woona za ntchito ya mdulidwe muunduna…
Read More » -
Mulanje yadya wani pa chitukuko
Boma la Mulanje ladya wani pogwiritsa ntchito ndalama za thumba la chitukuko m’dera la phungu la Constistuency Development Fund (CDF),…
Read More » -
Chimanga kulibe amalawi adandaula ndi Admarc
Pamene njala ikupitirira kukantha m’madera ena, zadziwikanso kuti m’misika ya Admarc yambiri m’dziko muno mulibe chimanga ndipo anthu ku Ntcheu,…
Read More » -
Kwaipa ku chipatala, mankhwala atha
Mwa mankhwala 100 amene amayenera kupezeka m’zipatala za boma, asanu okha ndiwo alipo, Nduna ya Zaumoyo Catherine Gotani-Hara idatero ku…
Read More » -
Aphungu apane boma posakaza chuma
Pamene aphungu a ku Nyumba ya Malamulo ayambe kukumana pa 8, mkulu wa bungwe loona zachilungamo pachuma la Malawi Economics…
Read More »