Tuesday, August 9, 2022
  • About Us
  • ImagiNATION
  • Rate Card
  • Contact Us
The Nation Online
Advertisement
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation
No Result
View All Result
No Result
View All Result
Home Chichewa

Agwiriridwa ali mtulo

by Martha Chirambo
30/08/2020
in Chichewa
2 min read
0
Share on FacebookShare on TwitterShare on WhatsAppShare on LinkedinLinkedinShare via Email

Pali zina zikamachitika, sungamvetse kuti zakhala bwanji. Mtsikana wina wa zaka 18 yemwe ali pabanja wagwiriridwa ali mtulo kumalo owedzera nsomba a Khuni, ku Dwangwa, m’boma la Nkhotakota.

Mtsikanayu adagwiriridwa pomwe naye mwamuna wake adali mtulo tofa nato pambali pake.

“Ndinkalota ndi kugona ndi munthu, ndipo nditadzidzimuka, ndidapezadi kuti ndikugona ndi munthu,” mtsikanayu adauza bwalo la milandu la

Nkhunga, m’bomalo.

Mtsikanayo akuti ankaganiza kuti munthuyo adali mwamuna wake koma adadabwa atanunkhiza mowa ndipo adazindikira kuti ankagwiriridwa chifukwa mwamuna wake samwa mowa komanso apa ndi pomwe adaona kuti mwamuna wake adali mtulo tofa nato pambali pake.

Apatu mpomwe adakuwa ndipo anthu adamugwira wogwirirayo ndi kupita naye kupolisi komwe adamutsekulira mlandu wogwiririra mosemphana ndi gawo 133 la malamulo a dziko lino.

Polankhulapo, mneneri wa polisi ya Khunga, Ignatius Esau adati udali usiku wa pa 16 August pomwe Raphael Kasakula wa zaka 21, adakalowera

m’nyumba banjalo   ndi kugwirira mayi wa m’nyumbamo.

Esau adati Kasakula yemwe ali ndi mkazi komanso ana awiri adauza bwalo la milandu la Nkhunga Lachisanu sabata yatha kuti mowa ndi omwe udamuchimwitsa.

“Kafukufuku wathu ngati apolisi udaonetsa kuti padalibe ubwenzi ulionse wa mseri pakati pa awiriwo koma kuti Kasakula adali mnzake wa mwamuna wa mtsikana yemwe adamugwirirayo,” adatero Esau.

Iye adati, koma anthu adadabwa kuti nkhaniyi ili ku bwalo la milandu, banjalo lomwe ndi asodzi, lidapempha a bwalo kuti atseke mlanduwu chifukwa Kasakula ndi mnzawo.

Koma woweruza milandu pakhotilo, Kingsley Buleya, adampeza Kasakula wolakwa pamlandu wogwiririra ndipo adamugamula kukakhala kundende kwa zaka 6.

Previous Post

‘Kudali ku Spar ya ku City Centre’

Next Post

Chisale threatens to sue for contempt

Related Posts

Patrick sakubwerera mmbuyo pa chikopa
Nkhani

Patrick Mwaungulu ndi katakwe pokankha chikopa

July 24, 2022
Chilima: Change the mindset toward development
Nkhani

A Chilima abwera poyera

July 1, 2022
Nkhani

Achilima awachepetsera mphamvu zaulamuliro

June 24, 2022
Next Post

Chisale threatens to sue for contempt

Opinions and Columns

My Turn

Bitcoin and regulations

August 8, 2022
Editor's Note

My beautiful experience as an intern

August 7, 2022
Editor's Note

My beautiful experience as an intern

August 7, 2022
Big Man Wamkulu

What is he up to? He doesn’t drink

August 7, 2022

Malawi-Music.com Top10

Trending Stories

  • Macra ordered MultiChoice Malawi not to 
implement the new proposed tariffs

    Court rebuffs MultiChoice Malawi on new tariffs

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Treasury Secretary says won’t resign

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Judiciary under probe 

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Chakwera’s austerity measures questioned

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Nankhumwa rally irks DPP governor

    0 shares
    Share 0 Tweet 0

  • Values
  • Our Philosophy
  • Editorial policy
  • Advertising Policy
  • Code of Conduct
  • Plagiarism disclaimer
  • Disclaimer
  • Privacy Policy
  • Terms of use

© 2022 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

No Result
View All Result
  • Home
  • News
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Life & Style
    • Every Woman
      • Soul
      • Family
    • Religion
    • Feature
  • Society
  • Columns
  • Sports
  • Chichewa
  • Enation

© 2020 Nation Publications Limited. All Rights Reserved.

This website uses cookies. By continuing to use this website you are giving consent to cookies being used. Visit our Privacy and Cookie Policy.