-
Chichewa
Pac ifuna mayankho pa za kukwera kwa mitengo
Kukwera kwa zinthu m’dziko muno kwaika Amalawi pamoto wa mavuto zomwe zachititsa kuti bungwe la Public Affairs Committee (PAC)…
Read More » -
Chichewa
Chikondi chiphetsa amuna awiri
Nthawi zina chikondi chikafikapo, chimazunguza mutu. Amuna awiri m’maboma a Machinga ndi Zomba adzikhweza sabata yathayi nkhani ya chikondi…
Read More » -
Nkhani
Asimbe lokoma ndani?: Civo, Manoma aswana mu Standard Bank
Pali ntchito mawa pabwalo la Civo mumzinda wa Lilongwe pamene timu ya Civo United ichapane ndi Mighty Be Forward…
Read More » -
Nkhani
Mafumu ‘okwatitsa’ ana athothedwa
Kachindamoto achotsa mafumu anayi Ana 549 abwerera kusukulu ku Dedza Kampeni yothamangitsa ana kubanja kuti abwerere kusukulu yafika pagwiritse m’boma…
Read More » -
Nkhani
Malamulo a ukwati akutsutsana
Kutanthauzira lamulo lokhudza maukwati a ana kukhala kovuta tsopano pamene pali kusemphana pakati pa zomwe zidalembedwa m’malamulo oyendetsera adziko lino…
Read More » -
Agumula chiliza nkutengamo alubino
Adaikidwa m’manda pa 27 May m’chaka cha 2000. Koma zodabwitsa zachitika pa 17 October 2015 pamene anthu olusa agumula…
Read More » -
Chichewa
Mwambo wa maliro wasintha ku CoM
Sukulu ya zaudotolo ya College of Medicine (COM) yasintha momwe mwambo wa maliro panyumba ya chisoni ya pasukuluyo mumzinda…
Read More » -
Nkhani
Kalikiliki popewa ngozi za madzi
Pamene nkhani yolosera mvula ili mkamwamkamwa, boma lati lili pakalikiliki kuti madzi osefukira amene amasautsa m’madera ena chaka chino lisakhale…
Read More » -
Nkhani
Moto lawilawi mu TNM Super League
Ligi ya TNM yafika pa lekaleka pamene matimu ena akutenga mapointi ndipo ena kutaya mwachibwana pamene ligiyi tsopano yalowa sabata…
Read More » -
Chichewa
‘Kudali ku mapemphero a Scom’
Patha zaka zisanu tsopano Dyson Milanzie yemwe ndi mkonzi wa mapologalamu kuwailesi ya kanema ku MBC-TV ali pabanja ndi njole…
Read More » -
Chichewa
Kwaterera kwa ntenje
Mwanunkha m’mudzi mwa Ntenje kwa T/A Machinjiri m’boma la Blantyre komwe osungitsa chitetezo m’midzi (community police) adatibulidwa n’kumangiriridwa pamtengo…
Read More » -
Chichewa
Boma lititeteze, atero achitetezo
Anthu okhwimitsa chitetezo m’mudzi mwa Ntenje, m’dera la T/A Machinjiri m’boma la Blantyre, apempha boma kuti liwateteze ndi kuwasamala…
Read More » -
Nkhani
Nanawa: Mlowam’malo wa kupitakufa
Matenda a HIV/Edzi asokoneza miyambo ina monga mwambo wa kupitakufa, womwe umapereka mphamvu kwa ‘fisi’ kuti akakonze maliro pocheza…
Read More » -
Chichewa
Ulangizi wabala mwana ku Mulanje
Njala yomwe yakhudza madera ambiri ikuvutanso m’boma la Mulanje komwe anthu akuyembekezereka kutuwa chifukwa cha mvula yanjomba yomwe adalandira…
Read More » -
Chichewa
Ntchito yasowa, wayamba ulimi wa kabichi
Adabwera m’tauni ya Blantyre kudzasaka ntchito atamaliza Fomu 4. Adaponda paliponse kukasaka ntchito, makalata chilembelenicho ndi satifiketi yake ya…
Read More » -
Man arrested for illegal possession of pistol, ammunition
Bangwe Police in Blantyre last Friday arrested 28-year-old Alex Matukuta of Sakwata Village, Traditional Authority (T/A) Nkalo in Chiradzulu for…
Read More » -
Nkhani
Flames inyamuka mawa
Timu ya Flames ikunyamuka mawa m’dziko muno ulendo ku Tanzania kukaswana ndi timuyi masewero amene alipo Lachitatu pa 7…
Read More » -
Nkhani
Bullets iphana ndi Wanderers lero
Ambiri adakamba kuti mwina masewero a lero pakati pa Bullets ndi Wanderers mu TNM Super League alephereka ponena kuti osewera…
Read More » -
Nkhani
Namrukhunua: Nyumba ya chilhomwe
Kalelo makolo adali ndi njira zawo zochitira zinthu kuti azisangalala ndi kukhala wotetezedwa. Alhomwe nawo ali ndi zimene makolo awo…
Read More » -
Nkhani
Mswati adakali mfumu—Boma
Boma, kudzera mwa mneneri wa unduna wa maboma aang’ono ke Muhlabase Mughogho, lati ngakhale pali kukokanakokana pa ufumu wa Gomani…
Read More »