Chichewa
-
Chakwera akwanitse malonjezo—HRDC
Bungwe la Human Rights Defenders Coalition (HRDC) lati maso ake akadali otsegula n’cholinga choti boma la Tonse Alliance lisaphwanye ufulu…
Read More » -
Masankhidwe a nduna autsa mapiri pa chigwa
Mtsutso wabuka ndi mmene mtsogoleri wa dziko lino, Lazarus McCarthy Chakwera, wasankhira nduna za boma lake. Amalawi ena akuti sakuonapo…
Read More » -
Malonjezo ayamba kuoneka
Boma latsopano la Tonse Alliance layamba kukwaniritsa ena mwa malonjezo ake a panyengo ya kampeni ndipo pomwe akadaulo osiyanasiyana ayamikira…
Read More » -
Maudindo ayamba kuchucha m’boma
Pomwe mtsogoleri wa dziko lino yemwe wangosankhidwa kumene Lazarus Chakwera wayamba kusankha adindo m’bom, ku Nyumba ya Malamulo zinthu zasadabuzika.…
Read More » -
Ulimi wa mthirira n’chuma
Tikudziweni… Ndine Moffat Mtalimanja ndipo ndi mkazi wanga Effie timachokera m’mudzi wa Kaunde, ku Namadidi kwa Senior Chief Mlumbe m’boma…
Read More » -
Mthirira usathere panjira
Kaitane Shuga wa m’mudzi mwa a Gavi ku Chileka m’boma la Blantyre ndi mmodzi mwa alimi amene amachita ulimi wothirira…
Read More » -
Chakwera wakwera
Pamene Amalawi amayembekezera bungwe lachisankho kuti lilengeze zotsatira za chisankho cha mtsogoleri wa dziko lino chimene chidachitika Lachiwiri pa 23…
Read More » -
Akhazikitsa kamtengo pachipatala cha nkhalamba
Malingana ndi kuchuluka kwa anthu achikulire amene amabwera pachipatala cha anthu okalamba cha Kalibu Elderly Clinic ku Lirangwe m’boma la…
Read More » -
Takonzeka kuvota—Amalawi
Pamene kwangotsala masiku awiri kuti Amalawi 6.8 miliyoni aponye voti yosankha mtsogoleri wa dziko lino, Amalawi ena asonyeza chidwi kuti…
Read More » -
Atsogoleri akwangula kampeni lero
Migwirizano ya zipani pachisankho chikudzachi zikuomba mkota wa mfundo za kampeni lero ndipo atsogoleri a m’migwirizanoyo akhala ali mbweee! kutolera…
Read More »