Chichewa
-
Ampingo avula gule zigoba
Madzi achita katondo kwa Kansonga m’dera la mfumu Chilowoko, m’boma la Ntchisi komwe Akhristu a mpingo wa CCAP wa Biwi…
Read More » -
Phindu lochuluka mu ng’ombe za nyama
Ngakhale ulimi wa ng’ombe za nyama umafuna mpamba wochuluka komanso phindu lake limabwera mochedwa, akadaulo a zaulimi wa ziweto akuti…
Read More » -
Zipani zakonzeka kusankha makomishona
Mtsogoleri wa dziko lino Peter Mutharika wauza zipani za ndale komanso nthambi yoyang’anira ogwira ntchito makhoti (Judicial Service Commission) kuti…
Read More » -
Covid-19 yakolera
Chiwerengero cha Amalawi amene apezeka ndi kachirombo ka coronavirus chatumphuka m’sabata ikuthayi kuchoka pa 101 kufika pa 203. Izi zachitika…
Read More » -
Mkokemkoke patsiku la chisankho
Zipani zotsutsa boma zalembera bwalo la milandu la Supreme Court kuti lifotokoze bwino pa za yemwe akuyenera kusankha tsiku loti…
Read More » -
APM alola ansah achoke
Mtsogoleri wa dziko lino Peter Mutharika dzulo wavomereza kuti wapampando wa bungwe la zisankho la Electoral Commission (MEC) Jane Ansah…
Read More » -
Chipwirikiti pachisankho
Pali chipwirikiti pachisankho cha mtsogoleri wa dziko lino, pomwe wapampando wa bungwe la zisankho la Malawi Electoral Commission (MEC) Jane…
Read More » -
Andale agundika misonkhano, osapewa Covid-19
M’sabatayi, anthu ena 5 adapezeka ndi kachirombo ka coronavirus m’dziko muno, kuchititsa kuti chiwerengero cha anthuwo chifike pa 63. Chiopsezo…
Read More » -
Chisankho chiliko
Bwalo lalikulu la milandu la Supreme Court dzulo lidagamula kuti bwalo lapadera la Constitutional Court (ConCourt) silidalakwe pogamula kuti chisankho…
Read More » -
Teketeke popereka zikalata
Mzinda wa Blantyre mudali teketeke m’sabatayi pomwe bungwe la zisankho la Malawi Electoral Commission (MEC) lidalandira zikalata za omwe akufuna…
Read More »