Chichewa
-
Ndale zimasokoneza ntchito zathu—MPS
Malawi Police Service (MPS) yavomera kuti mmbuyomu imalephera kugwira ntchito zawo mwaukadaulo kaamba ka andale omwe amalowerera kwambiri pa ntchito…
Read More » -
Fisi wadya mayi wa ku Tsangano
Anthu a m’mudzi mwa Doviko, Mfumu Mpando, m’boma la Ntcheu, akukhala ndi mantha chifukwa cha afisi omwe akuzunguza m’deralo. Loweruka…
Read More » -
Mzomera wadzipereka m’manja mwa apolisi
Gavanala wa chipani cha Democratic Progressive Party (DPP) m’chigawo chakumpoto Christopher Mzomera Ngwira wadzipereka m’manja mwa apolisi Lachinayi. Mzomera, yemwe…
Read More » -
Kainja wadza ndi lumo lakuthwa
Mkulu wapolisi George Kainja wati adzutsa milandu yonse yogonera n’cholinga chopereka chikhulupiriro mwa Amalawi chokhudza apolisi. Pocheza ndi wailesi ya…
Read More » -
Chisale watuluka n’kumangidwanso
Mawu a wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino, Saulos Klaus Chilima, womwe amauza anthu m’misonkhano yake ya kampeni kuti adzakwizinga…
Read More » -
Sipakala waimitsa Nyumba ya Malamulo
Sipikala waimitsa Nyumba ya Malamulo kwa sabata ziwiri kaamba ka phungu ndi ogwira ntchito ena ku nyumbayi omwe akhudzidwa ndi…
Read More » -
Pa Wenela pasintha zedi
Tsikulo pa Wenela padali fumbi. Lazalo Watsika wabwera ndi moto ndithu. “Abale inu, dzikotu ili limatembenuka zedi. Ndani ankadziwa kuti…
Read More » -
ANatchereza
Sakufuna kukaonekera Gogo Natchereza, Mnyamata wina adandifunsira chibwenzi ndi cholinga choti tidzakwatirane. Padakali pano padutsa zaka zinayi tili paubwenzi, koma…
Read More » -
Tidakumana ku sukulu ku Chiradzulu
Gift Banda ndi mkazi wake Tisunge Mandala adakumana koyamba ali ku sukulu ya sekondale ya Chiradzulu komwe ankaphunzira. Atatsiriza maphunziro…
Read More » -
Bishopu aganiziridwa kugwiririra mwana
Madzi achita katondo pa mpingo wa Assemblies of Fountain ku Chileka m’boma la Lilongwe komwe bishopu wa mpingowu Alexander Selemani…
Read More »