Nkhani
-
Kachali apepesa: Kulankhula motumbwa kuthe
Anthu, a mabungwe omwe siaboma, katswiri pandale kudzanso mfumu ina ati andale asamaledzere ndi maudindo n’kufika poiwala kulemekeza anthu omwe…
Read More » -
Nigeria, Malawi agwilana manja
Pamene dziko la Malawi lili mkati mwazokambirana ndi dziko la Tanzania pa nkhani ya umwini wa nyanja ya Malawi yomwe…
Read More » -
Amalawi akulira ndi kukwera kwa mafuta
Mkulu wa bungwe loona za ufulu wa ogula malonda la Consumers Association of Malawi (CAMA), John Kapito, wati boma lichite…
Read More » -
Zochitika ku mwambo wa kulamba
Loweruka lapitalo kudali chaka ku likulu la mfumu yaikulu ya Achewa m’maiko a Malawi, Zambia ndi Mozambique Kalonga Gawa Undi…
Read More » -
‘Kusowa kwa mpikisano n’kwachabe’
Pali mantha kuti zipani za m’dziko muno zingayoyoke ngati makatani ngati mipando yonona yachipani monga wa pulezidenti ndi wachiwiri wake…
Read More » -
Alendo alanda maudindo mu PP
Kusankhidwa kwa ‘alendo’ ochoka m’zipani zina kukhala m’maudindo onona kuchipani cholamula cha People’s (PP) kungakolezere mavuto kuchipaniko, maka pandawala yolowera…
Read More » -
Moto utentha misika, njakata izinga
A malonda omwe katundu wawo adapsera m’misika ya mavenda ya Tsoka ku Lilongwe komanso wa Blantyre akulira chokweza, uku akupempha…
Read More » -
Kudziwa za m’thupi; kukonza tsogolo
Sabata yatha inapatulidwa ndi boma pankhani yoyezetsa magazi kuti anthu adziwe ngati ali ndi kachirombo koyambitsa Edzi ka HIV. Mutu…
Read More » -
Akufuna wogwirizira ufumu achoke, apepese
Mafumu m’dziko muno agwirizana ndi ganizo la mtsogoleri wa dziko lino Joyce Banda kuti magulupu ndi nyakwawa asiye kulandirira ndalama…
Read More » -
Moto wayaka ku Nkosini
Pasanadutse n’komwe mwezi chilongere Inkosi Yamakosi Gomani Yachisanu ku Ntcheu, fumbi labuka pomwe mbali ina kubanjalo ikukakamiza wogwirizira, Rosemary Malinki…
Read More » -
Mswati akhale chitsanzo kwa achinyamata
Pulezidenti Joyce Banda wati mfumu yachingoni yomwe angoidzoza kumene, Mswati Kanjedza Gomani yachisanu ikhale chitsanzo kwa achinyamata. Banda amalankhula izi…
Read More » -
Kuyezetsa magazi kwayenda bwino
Mlembi wamkulu mu Unduna wa Zaumoyo wati sabata yolimbikitsa kuyezetsa magazi pofuna kudziwa ngati uli ndi kachilombo koyambitsa Edzi idali…
Read More » -
Akufuna lamulo lothana ndi uchidakwa
Unduna wa zaumoyo wati ukukonza lamulo lomwe cholinga chake n’kulonderapo pa kamwedwe kamowa m’dziko muno. Woyang’anira za matenda osapatsirana muundunawu…
Read More » -
Amalawi akulira, chitetezo chachepa
Akuluakulu a mabungwe omwe siaboma ati kuchepa kwa malipiro a apolisi ndi chimodzi mwa zomwe zalowetsa pansi chitetezo m’dziko muno…
Read More » -
Achotsa mavenda popanda ziwawa ku Lilongwe
Kunali njinga yapulula machaka ku Lilongwe Lachisanu lapitalo pomwe anthu mazanamazana amabwerera m’makwawo opanda kanthu m’manja atalephera kukolola posalima akuluakulu…
Read More » -
DPP idzudzula boma
Chipani chakale cholamula cha Democratic Progressive (DPP) chati Amalawi angapitirire kusauka ngati boma la chipani cha People’s (PP) silibwera msanga…
Read More » -
Kusanthula ulamuliro m’masiku 100 a Banda
Boma la mtsogoleri wa dziko lino, Joyce Banda, likuyenera kukhwimitsa chitetezo m’dziko muno, kuchepetsa kumanga anthu chisawawa komanso kuchepetsa kuchotsa…
Read More » -
Chitetezo chachepa, tithandizeni—anthu
Anthu m’dziko muno apempha boma kuti lichite changu pobwezeretsa chitetezo chomwe ati chalowa libolonje m’masiku apitawa. Izi zalankhulidwa m’kati mwa…
Read More » -
Gawo 65 yazunguzanso mitu aphungu
Mpungwepungwe wabukanso ku Nyumba ya Malamulo pomwe pali kuponyerana Chichewa pakati pa aphungu achipani cha DPP ndi aphungu omwe adachoka…
Read More » -
‘Bingu adafa bwanji, pakhale kafukufuku’
A mabungwe omwe si a boma, mfumu ina yaikulu komanso anthu angapo otumikiridwa ati n’koyenera kuti Amalawi adziwe bwino lomwe…
Read More »