Chichewa
-
Bajeti iganizire mavuto a anthu
Ndondomeko ya chuma ndiyo chiyembekezo chachikulu tsopano chomwe chingachepetse mavuto omwe anthu akukumana nawo kaamba ka kukwera mitengo ya zinthu…
Read More » -
Apolisi anjatidwa pokhudzidwa ndi ophedwa pa zionetsero
Apolisi asanu ndi anayi adatengedwa m’sabatayi powaganizira kuti akudziwapo kanthu pa za ena amene adaphedwa pazionetsero za pa 20 Julaye…
Read More » -
‘Boma likweza malipiro’
Ogwira ntchito angasimbe lokoma ngati ganizo la unduna wa zantchito lokweza malipiro otsikitsitsa amene amalandira lingafitsidwe. Izi zadza ogwira ntchito…
Read More » -
Konvenshoni ya MCP yalephereka
Chipani cha Malawi Congress Party (MCP) chati msonkhano wake waukulu wa konvenshoni umene umayenera kukhalapo pakati pa lero ndi Lolemba…
Read More » -
Zipolowe zikuphulika
Pamene tikuyandikira chaka cha 2014 pomwe Amalawi akuyembekeza chisankho cha magawo atatu chosankha Pulezidenti, aphungu a Kunyumba ya Malamulo ndi…
Read More » -
Wailesi ya Dzimwe ikusowa thandizo ku Mangochi
Nyumba youlutsira mawu ya Dzimwe Community Radio ku MonkeyBay m’boma la Mangochi yapempha thandizo lomangira ofesi komanso kugula zida zoulutsira…
Read More » -
Konvenshoni ya MCP pa 28 April
Pamene chipani cha Malawi Congress Party (MCP) chatsimikiza kuti msonkhano wake waukulu wokasankha atsogoleri udzachitika pa 28 ndi 29 Epulo,…
Read More » -
Olephera asatuluke DPP—Mutharika
EMMANUEL MUWAMBAYemwe anali mtsogoleri wogwirizira mpando wa pulezidenti wa chipani cha DPP, Peter Mutharika, Lachinayi adalangiza omwe amapikisana nawo pofuna…
Read More » -
Tikolola chimanga chochuluka—Nduna
Nduna ya zamalimidwe komanso kuonetsetsa kuti m’dziko muno muli chakudya chokwanira, Peter Mwanza yati undunawu ukulosera kuti chaka chino dziko…
Read More » -
Amayi omwe ali ndi kachilombo akufuna mudzi wawo
Amayi omwe ali ndi kachilombo koyambitsa matenda a Edzi ka HIV kwa T/A Kalolo ku Lilongwe apempha boma kuti liwapatse…
Read More »