Chichewa
-
Apolisi aphunzira kagwiridwe ka ntchito yawo
Polisi ya Nkhotakota yakhala yoyamba kuphunzitsidwa za momwe angagwirire ntchito yawo panthawi ya zipolowe komanso zionetsero. Maphunzirowa akudza poyang’anira chisankho…
Read More » -
‘BAMBO ATHOTHA MWANA’
Bambo wina m’mudzi mwa Nchada kwa T/A Nthondo ku Ntchisi amulamula kuti alipe mkazi wake ndi mwana wake wamkazi wa…
Read More » -
Kudziongola ngati zenizeni, koma ayi
Lachitatu sabata yatha anyamata a Flames, ngakhale adapeza mwayi wochuluka kuposa Namibia, adalepherana ndi timuyo mumpikisano wolimbirana malo ku mpikisano…
Read More » -
Woba chiponde ku Chiladzulu agwidwa
Bwalo la Chiradzulu layamba kuzenga mlandu Operations Manager wa kampane yolondera ya Global Communications Centre pomuganizira mlandu woba chiponde cha…
Read More » -
Mkulu wa kunyumba ya chisoni agwidwa ndi ziwalo
Abambo awiri omwe amagwira ntchito kunyumba yachisoni kuchipatala cha Kamuzu Central (KCH) akuzengedwa mlandu wodula maliseche a mtembo wa munthu…
Read More » -
‘Wogona’ ndi mwana wake pofuna mfumba agwidwa
Ndani adanena kuti chizimba cha mfumba ndi kugona ndi mwana wako? Izi zachitika ku Dedza komwe apolisi anjata bambo wa…
Read More » -
Mpingo ukana mbusa womangidwa za zitupa
Mpingo wa Lord’s Chosen Charismatic Revival Ministries (LCCRM) wakana zomwe munthu wina wa ku Cameroon adauza nthambi yoona za anthu…
Read More » -
Amayi abisa katundu wa K16 000 mu panti
Ukathyali wakasololedwe wachitika pamalo omwetsera mafuta a Puma pa Wenela pomwe apolisi adanjata mkulu wina wa ku Zambia pomuganizira kuti…
Read More » -
Maneb ikhutila ndi mayeso a sitandade 8
Bungwe loyendetsa mayeso la Malawi National Examinations Board (Maneb) lati lakhutira ndi mmene mayeso a Sitandade 8 ayambira. Mkulu wa…
Read More » -
Anthu a ku Likoma alirira Ilala
Anthu okhala pazilumba za Likoma ndi Chizumulu ati akulira ndipo moyo ukutentha chifukwa cha kusiya kuyenda kwa sitima ya Ilala.…
Read More »