Chichewa
-
Chisankho chanunkhira, koma ku MCP kuli chuuu!
Pamene anthu m’madera ena ayambe kulembetsa maina awo m’kalembera wa chisankho cha magawo atatu cha chaka chamawa Lolemba likudzali, sizidadziwikebe…
Read More » -
Malawi wapindulanji muzaka 49?
Pamene dziko lino lero likukumbukira kuti lakwanitsa zaka 49 lili pa ufulu wodzilamulira, Amalawi ena ati ngakhale pali zina zolozeka…
Read More » -
Aphunzitsi adzawalabadire ndani?
Ambiri timadzudzula kujombajomba komanso kusalimbikira ntchito kwa aphunzitsi m’sukulu za boma. Mchitidwewu ngopititsa pansi maphunziro chifukwa ophunzira amachoka kusukulu asanasulidwe…
Read More » -
Scova adatani?
Nkhani yavuta m’sabatayi ndi ya Nyerere kuti zidagenda pomwe zimasewera ndi Blue Eagles. Aganyu sitivomereza kugenda ndipo tafuna timvetsetse chomwe…
Read More » -
Ntchito yomanga njanji iima
Ntchito yomanga njanji yochoka ku Kachaso kupita ku Nkaya ayiimitsa mpaka kampani ya Mota-Engel ndi ogwira ntchito kukampaniyo atamvana chimodzi.…
Read More » -
Mandela adwala mwa kayakakaya ku South Africa
Mtsogoleri wakale wa dziko la South Africa Nelson Mandela adali kudwalika zedi pachipatala china ku Pretoria m’dzikomo. Pomwe timasindikiza Tamvani…
Read More » -
‘Lamulo la chuma cha pulezidenti liunikidwenso’
Mmodzi mwa akatswiri a za malamulo Edge Kanyongolo wati lamulo lomwe likukamba za katundu ndi chuma cha atsogoleri a dziko…
Read More » -
Mayi athokoza ataomboledwa
Maness Thom wa Zaka 65 wathokoza bungwe losakhulupirira kuti kunjaku kuli Mulungu komanso mphamvu za mizimu ina la Association of…
Read More » -
Wa zaka 70 wofuna kugwiririra amangidwa
Bwalo lamilandu la Dedza Lachiwiri lagamula gogo wa zaka 70 kuti akaseweze kundende zaka zinayi kaamba kofuna kugwiririra mdzukulu wake…
Read More » -
Nanga wapolisi ataphofomoka?
Masiku ano sichikhala chachilendo kuona apolisi atakwera galimoto mosayenera. Ngakhale ntchito yawo n’kuonetsetsa kuti malamulo akutsatidwa, ngakhale pamsewu, apolisiwo ndiwo…
Read More »