Nkhani

Nanga wapolisi ataphofomoka?

Listen to this article

Masiku ano sichikhala chachilendo kuona apolisi atakwera galimoto mosayenera. Ngakhale ntchito yawo n’kuonetsetsa kuti malamulo akutsatidwa, ngakhale pamsewu, apolisiwo ndiwo amakhala oyamba kuphwanya malamulowo. Kodi anthu wamba atakwera galimoto monga achitira apa apolisi, sangakalowe kozizira? Mwinatu iwowa ali ndi mphamvu kuposa lamulo.

Uku kudali kumpira wa Malawi ndi Kenya Lachitatu ku Kamuzu Stadium mumzinda wa Blantyre. Chomwe chimadabwitsa n’chakuti nanga ataphofomoka pa galimotoyo, olakwa akuwathamangitsawo angagwidwe ndi ndani?

Related Articles

Back to top button