Nkhani
-
Njira yatsopano yotololera misonkho yautsa mapiri pa chigwa
Sitolo m’madera ambiri makamaka m’mizinda ikuluikulu zakhala zotseka mkati mwa sabatayi pomwe eni sitolozo sakugwirizana ndi njira yatsopano yotolera misonkho…
Read More » -
Amalawi akulira ndi vuto la magetsi
Amalawi akudandaula usiku ndi usana kaamba ka kuthimathima kwa magetsi komwe akuti kwasokoneza mabizinesi ndi mabajeti m’mabanja chifukwa ena akuopa…
Read More » -
Ng’ona zavuta zedi ku Nsanje
Anthu okhala m’midzi ya m’madera a T/A Katunga, Kasisi komanso Mulilima m’boma la Chikwawa ati miyoyo yawo ili pa chiopsezo…
Read More » -
Akaniza belo, DNA kwa a Malemia
Bwalo la milandu ku Zomba lakana kupereka belo kwa Senior Chief Malemia komanso kuyeza DNA kuti adziwe mimba imene mfumuyo…
Read More » -
Kulibe kuzondana kaamba ka kusowa kwa mafuta
Amalawi tsopano ayamba kulingalira mozama asadapange ulendo kuopa kuti angakwangule konse kamthumba komwe khomo likuyang’anira pa zosowa zonse kaamba ka…
Read More » -
Chikho cha fodya chasefuka
Chikho cha fodya chaka chino chasefukira ndi makilogalamu 27 miliyoni zomwe zabweretsa nkhawa yoti mtengo wake ukhoza kukhala wonyotsolera ku…
Read More » -
Akhazikitsa ndondomeko za CDF
Unduna wa maboma ang’onoang’ono wati makhonsolo ndi okonzeka kuyendetsa thumba la ndalama za chitukuko la CDF pogwiritsa ntchito ndondomeko zomwe…
Read More » -
Mlandu wa a Malemia ukupitirira mawali
Bwalo la milandu la Zomba Senior Resident Magistrates Court kuyambira 8 koloko mawa lino lipitiriza kumva mlandu wa a Senior…
Read More » -
Amalawi akufinyika
Pamene mtengo wa mafuta udakwera Lachitatu sabata ikuthayi, Amalawi ochokera m’madera osiyanasiyana m’dziko lino ati kulira n’kosayamba. Koma ikakuona litsiro…
Read More » -
Ana 63 mwa 100 akukwapulidwa
Makolo ena ati ndi wokondwa ndi mfundo yoti pakhale chilango chokhazikika kwa aphunzitsi amene angapezeke akumenya ophunzira. Komiti yoona za…
Read More »