Nkhani
-
Zaka zitatu kwa wogona ndi mbuzi
Bwalo la milandu la First Grade Magistrate la Nkhunga m’boma la Nkhotakota, lagamula a Sandram Lyson, omwe ndi a zaka…
Read More » -
A Mpesi atula pansi udindo
Pomwe kwatsala masiku 30 enieni kuchoka lero kuti chisankho chapadera m’madera angapo chidzachitike, mkulu woyendetsa zisankho ku bungwe la Malawi…
Read More » -
When mob justice myths leave trail of blood
Like any other day, dawn broke peacefully on Saturday, May 9, as 42-year-old Madalitso Joe William went about his daily…
Read More » -
Kafukufuku wa ndege wayamba
Amalawi tsopano maso ali gaaa pa komiti yapadera ya ku Nyumba ya Malamulo yomwe ikufufuzanso chomwe chidachititsa ngozi ya ndege…
Read More » -
Njira yatsopano yotololera misonkho yautsa mapiri pa chigwa
Sitolo m’madera ambiri makamaka m’mizinda ikuluikulu zakhala zotseka mkati mwa sabatayi pomwe eni sitolozo sakugwirizana ndi njira yatsopano yotolera misonkho…
Read More » -
Amalawi akulira ndi vuto la magetsi
Amalawi akudandaula usiku ndi usana kaamba ka kuthimathima kwa magetsi komwe akuti kwasokoneza mabizinesi ndi mabajeti m’mabanja chifukwa ena akuopa…
Read More » -
Ng’ona zavuta zedi ku Nsanje
Anthu okhala m’midzi ya m’madera a T/A Katunga, Kasisi komanso Mulilima m’boma la Chikwawa ati miyoyo yawo ili pa chiopsezo…
Read More » -
Akaniza belo, DNA kwa a Malemia
Bwalo la milandu ku Zomba lakana kupereka belo kwa Senior Chief Malemia komanso kuyeza DNA kuti adziwe mimba imene mfumuyo…
Read More » -
Kulibe kuzondana kaamba ka kusowa kwa mafuta
Amalawi tsopano ayamba kulingalira mozama asadapange ulendo kuopa kuti angakwangule konse kamthumba komwe khomo likuyang’anira pa zosowa zonse kaamba ka…
Read More » -
Chikho cha fodya chasefuka
Chikho cha fodya chaka chino chasefukira ndi makilogalamu 27 miliyoni zomwe zabweretsa nkhawa yoti mtengo wake ukhoza kukhala wonyotsolera ku…
Read More »