Nkhani
-
Amanga mayi pa mlandu wovulaza m’nzawo ku nkhope
A Police ku Neno amanga a Grace Samuel a zaka 33 kaamba kowaganizira kuti anavulaza mayi m’nzawo atamuthira madzi otentha…
Read More » -
Mayi wakakamira kuti mlandu wake uwerudzidwe, uthe
Mau aja amati kumayenda kuti uone agalu a michombo adapherezeka mkati mwa sabatayi pomwe mayi wina wa zaka 22 ku…
Read More » -
Aphungu ayembekezere mtsutso wokhetsa thukuta
Pomwe mkumano wa aphungu udayamba Lachiwiri pa 7 July, 2026, nkhani mkati mwa sabatayi zasonyeza kuti mbali yomwe siidakonzekere bwino…
Read More » -
Koma lipoti la hotela ya amaryllis lidzatuluka?
Chikaiko chayambanso kukula ngati lipoti la kafukufuku wa momwe hotela ya Amaryllis idagulitsidwira libwere mu Nyumba ya Malamulo pa mkumano…
Read More » -
Zaka zitatu kwa wogona ndi mbuzi
Bwalo la milandu la First Grade Magistrate la Nkhunga m’boma la Nkhotakota, lagamula a Sandram Lyson, omwe ndi a zaka…
Read More » -
A Mpesi atula pansi udindo
Pomwe kwatsala masiku 30 enieni kuchoka lero kuti chisankho chapadera m’madera angapo chidzachitike, mkulu woyendetsa zisankho ku bungwe la Malawi…
Read More » -
When mob justice myths leave trail of blood
Like any other day, dawn broke peacefully on Saturday, May 9, as 42-year-old Madalitso Joe William went about his daily…
Read More » -
Kafukufuku wa ndege wayamba
Amalawi tsopano maso ali gaaa pa komiti yapadera ya ku Nyumba ya Malamulo yomwe ikufufuzanso chomwe chidachititsa ngozi ya ndege…
Read More » -
Njira yatsopano yotololera misonkho yautsa mapiri pa chigwa
Sitolo m’madera ambiri makamaka m’mizinda ikuluikulu zakhala zotseka mkati mwa sabatayi pomwe eni sitolozo sakugwirizana ndi njira yatsopano yotolera misonkho…
Read More » -
Amalawi akulira ndi vuto la magetsi
Amalawi akudandaula usiku ndi usana kaamba ka kuthimathima kwa magetsi komwe akuti kwasokoneza mabizinesi ndi mabajeti m’mabanja chifukwa ena akuopa…
Read More »