Nkhani
-
Alangiza aphungu achepetse tulo
Aphungu a ku Nyumba ya Malamulo adakwangula mkumano wawo sabata yatha atadutsitsa mabilu 14 omwe ambiri akukhudza za chuma ndi…
Read More » -
Amanga opezeka ndi mankhwala popanda chilolezo
Apolisi ku Mponela m’boma la Dowa amanga abambo atatu omwe adapezeka ndi mankhwala osiyanasiyana omwe amagulitsa mgolosale yawo. Mneneri wa…
Read More » -
‘Chikondi chizidutsa malire’
Chikondi chomwe chidayambira pa tsamba la pa Intaneti lofunafuna zibwenzi chasintha kukhala banja kwa mayi wa malonda a ku Malawi,…
Read More » -
Amanga a Chikomeni pa za chamba
Apolisi a kwa Jenda ku Mzimba Lachisanu adamanga a Ras David Chikomeni Chirwa, a zaka 49 powaganizira kuti adapezeka ndi…
Read More » -
Sitima za tsopano zidzafewetsa miyoyo
Anthu okhala mozungulira, komanso pa zisumbu m’nyanja ya Malawi; pamodzi ndi ochita malonda osiyanasiyana akuyembekezera ndi chidwi kupherezera kwa lingaliro…
Read More » -
Malemia amangidwa zaka 21
Bwalo la majisitileti ku Zomba lachisanu lidagamula Senior Chief Malemia kuti akakhale ku ndende zaka 21 pa mlandu wogonana ndi…
Read More » -
‘Mitengo yomangira ma CDSS yanyanya’
Nduna yoona za maphunziro a Bright Msaka achenjeza kuti ndalama zonse za m’thumba la chitukuko la Constituency Development Fund (CDF)…
Read More » -
Boma lapereka K100biliyoni yogulira chimanga
Nduna ya za chuma, mapulani a za chuma, komanso kupereka mphamvu ku anthu a Joseph Mwanamvekha yati boma lapereka K100…
Read More » -
Chipepeso kaye musanayambe mseu
Nzika zokhudzidwa ku Liwonde m’boma la Machinga zaopsedza kuti ziletsa kuyamba kwa ntchito yokonzanso msewu wa Liwonde-Matawale (M003) pokhapokha boma…
Read More » -
Amanga mayi pa mlandu wovulaza m’nzawo ku nkhope
A Police ku Neno amanga a Grace Samuel a zaka 33 kaamba kowaganizira kuti anavulaza mayi m’nzawo atamuthira madzi otentha…
Read More »