-
Chichewa
Ankadziwana ndi mayi anga’
Kale makolo amachita kusankhira ana awo munthu wokwatirana naye, koma pano zinthu zidasintha ngakhale kuti makolowo akhoza kungokhala muni…
Read More » -
Chichewa
Apumphuntha ana ndi nsimbi
Ana atatu a banja limodzi abwerera lokumbakumba mayi wawo Eveter Kulemera, wa zaka 24, akuti atawalumira mano kuwapumphuntha ndi…
Read More » -
Chichewa
Khama lipindula paulimi—Phungu
Nthawi zambiri chomwe chimasowa paulimi ndimasomphenya. Alimi ambiri amangolingalira zoti ndikakolola chaka chino ndidzalimanso chaka cha mawa mmalo moti azilingalira…
Read More » -
Chichewa
Chidyaabusa: Nthumbwana yofewetsetsa
Zamkati mwa nyama monga ng’ombe kapena mbuzi zija ena amati nthumbwana ndi ndiwo zofewa zomwe ambiri amakonda kupatsa mafumu kapena…
Read More » -
Chichewa
Ziweto zisasowe mtendere m’khola
yengo ya mvula ino, ziweto monga ng’ombe, mbuzi, nkhosa ndi nkhumba zimasauka kaamba ka matope m’khola, zomwe zimachititsa kuti…
Read More » -
Chichewa
Bungwe lilangiza alimi kubzala mbewu zopirira
Malingana ndi kabweredwe ka mvula ya masiku ano, akatswiri alimbikitsa kuti alimi asamangoganiza za mbewu zamakono koma mbewuzo zizikhala…
Read More » -
Chichewa
Tsogolo la fizi silikudziwika
Zenizeni pankhani yoti fizi yokwera m’sukulu za sekondale ndi sukulu za ukachechenjede za boma ipitilire kapena ayi zidziwika posachedwapa…
Read More » -
Chichewa
Alandira upangiri pa malonda a mbewu
Ochita bizinesi yogulitsa mbewu a m’maboma 7 m’dziko muno alandira upangiri wa momwe angapewere kuononga bizinesi yawo popezeka ndi…
Read More » -
National News
Lilongwe taps to be dry over festive season
Massive siltation of Lilongwe River, the main water source for Lilongwe Water Board (LWB) has led to a dive…
Read More » -
Chichewa
Zasokonekera ku kapitolo
Zili kukapitolo ku Lilongwe si ndizo. Pomwe apolisi achilimika kugwira ndi kutsekera galimoto zopezeka ndi milandu, oyendetsa minibasi agangalama…
Read More » -
Chichewa
The Rain: Mnyamata wanthetemya
Anthu ambiri otchuka makamaka amasewero, oyimba ndi azisudzo amakonda kudzitcha maina otchukira kusiya awo a pamchombo. Mchitidwewu sudayambire kuno…
Read More » -
Chichewa
Ngozi zanyanya chaka chino—Apolisi
Apolisi ati ngozi za pamsewu m’dziko muno zachuluka ndi 18 pa ngozi 100 zilizonse poyerekeza ndi chaka chatha nyengo…
Read More » -
Chichewa
Boma likonzekera el nino—chilima
Boma lati alimi ndi anthu m’dziko muno asanjenjemere ndi lipoti la nthambi ya zanyengo loti chaka chino kukhoza kukhala…
Read More » -
Chichewa
Bwanji nkhuku yoweta sagula pamsika?
Achewa ali ndi njira zosiyanasiyana zoperekera malango pakati pawo. Njira zina ndi monga nthano, magule, ndakatulo, chinamwali ndi miyambi ndi…
Read More » -
Chichewa
Msika wa zondeni ngosayamba
Katswiri wa zamadyedwe m’dziko muno, Chrispine Jedegwa, akupanga ndi kugulitsa ufa wa mbatata ya kholowa yamakolo yotchedwa zondeni yomwe…
Read More » -
Chichewa
Bzalani mbewu zocha msanga—Lipita
Woyendetsa ntchito za ulangizi ndi njira zamakono za ulimi muunduna wa zamalimidwe, Wilfred Lipita, wati alimi akuyenera kutengerapo phunziro…
Read More » -
Chichewa
Atukuka ndi kukwatitsa mitengo ya zipatso
Masiku ano nkhani ili mkamwamkamwa paulimi ndi yogwiritsa ntchito mitundu ya mbewu zamakono zomwe akatswiri adayesa n’kupeza kuti zili…
Read More » -
Chichewa
Khrisimasi ya maluzi
Kwangotsala masiku anayi kuti chisangalalo cha Khrisimasi chifike pachimake koma ochita bizinesi zosiyanasiyana akudandaula kuti sizikudziwika kuti nyengoyi yafikadi…
Read More » -
National News
Commissioner blasts corrupt traffic cops
Central Region Police commissioner George Kainja has said traffic police are denting the image of the Malawi Police Service…
Read More » -
Chichewa
Pewani chipalamba posamala mitengo
Kampani yogula fodya ya Limbe Leaf Tobacco Company yati makolo azitsogolera ana pantchito yobzala mitengo kuti m’dziko muno…
Read More »