-
Chichewa
Boma likonzekera el nino—chilima
Boma lati alimi ndi anthu m’dziko muno asanjenjemere ndi lipoti la nthambi ya zanyengo loti chaka chino kukhoza kukhala…
Read More » -
Chichewa
Bwanji nkhuku yoweta sagula pamsika?
Achewa ali ndi njira zosiyanasiyana zoperekera malango pakati pawo. Njira zina ndi monga nthano, magule, ndakatulo, chinamwali ndi miyambi ndi…
Read More » -
Chichewa
Msika wa zondeni ngosayamba
Katswiri wa zamadyedwe m’dziko muno, Chrispine Jedegwa, akupanga ndi kugulitsa ufa wa mbatata ya kholowa yamakolo yotchedwa zondeni yomwe…
Read More » -
Chichewa
Bzalani mbewu zocha msanga—Lipita
Woyendetsa ntchito za ulangizi ndi njira zamakono za ulimi muunduna wa zamalimidwe, Wilfred Lipita, wati alimi akuyenera kutengerapo phunziro…
Read More » -
Chichewa
Atukuka ndi kukwatitsa mitengo ya zipatso
Masiku ano nkhani ili mkamwamkamwa paulimi ndi yogwiritsa ntchito mitundu ya mbewu zamakono zomwe akatswiri adayesa n’kupeza kuti zili…
Read More » -
Chichewa
Khrisimasi ya maluzi
Kwangotsala masiku anayi kuti chisangalalo cha Khrisimasi chifike pachimake koma ochita bizinesi zosiyanasiyana akudandaula kuti sizikudziwika kuti nyengoyi yafikadi…
Read More » -
National News
Commissioner blasts corrupt traffic cops
Central Region Police commissioner George Kainja has said traffic police are denting the image of the Malawi Police Service…
Read More » -
Chichewa
Pewani chipalamba posamala mitengo
Kampani yogula fodya ya Limbe Leaf Tobacco Company yati makolo azitsogolera ana pantchito yobzala mitengo kuti m’dziko muno…
Read More » -
Chichewa
Alimi musaiwale mitengo ya chonde
Bungwe lomwe limalimbikitsa alimi kubzala mitengo yosiyanasiyana la World Agroforesry Centre lapempha alimi kuti asaiwale mitengo ya chonde akamabzala…
Read More » -
Chichewa
Kamatira: Nthenda yosautsa
Thenda zina ukazimva mmakutu kuchita kuwawa chifukwa chakuwopsa kwake. Anthu ambiri amataya mtima ndi matenda aja a Edzi komatu…
Read More » -
Chichewa
‘Olandira makuponi pano mu 2016 sadzalandiranso’
Boma lati kuyambira chaka chino, yemwe wapindula nawo mupologalamu ya zipangizo zaulimi zotsika mtengo ya Farm Input Subsidy Programme…
Read More » -
Chichewa
Akupha makwacha ndi zipatso
Chaima Banda, mlimi wa zipatso kwa Manondo, T/A Nkukula ku Lilongwe, akusimba lokoma ndi ulimi wake womwe wakhala akuchita…
Read More » -
Chichewa
Wagolosale ndiye adandipatsa nambala yake’
Anthuni, njira zophera khoswe n’zambiri koma chachikulu khosweyo afe basi. Ena pofuna mkazi amachita kugwa m’ngongole kuti aoneke ngati,…
Read More » -
Chichewa
GANIZO LOKWEZA FIZI LIBWERETSA NJIRIMBA
Kudali matatalazi ku Nyumba ya Malamulo Lachinayi lapitali pamene aphungu adapindirana ndevu mkamwa pokambirana za ganizo la boma miyezi…
Read More » -
Chichewa
Za ukamberembere mu Fisp akuti zichepe chaka chino
Ntchito yotumiza zipangizo zaulimi zotsika mtengo mupologalamu ya Farm Input Subsidy Programme (Fisp) ili mkati koma nyengo ngati iyi…
Read More » -
Chichewa
Ku Nkhoma sakugona ndi mthirira
Amati mmera mpoyamba. Ukalephera kukonzekera koyambirira ntchito yonse imayenda mwapendapenda mpaka zipatso zake zimakhala zokhumudwitsa. Ino ndi nyengo ya dzinja…
Read More » -
Chichewa
NG’AMBA IOPSEZANSO CHAKA CHINO—UNDUNA
Chaka chatha kudali kakasi pankhani ya ulimi mvula itadula pomwe mbewu zambiri, maka chimanga, zimamasula ndipo izi zidachititsa kuti…
Read More » -
Chichewa
Tetezani kukokoloka kwa nthaka ndi biyo
Njira zotetezera nthaka kumadzi othamanga zili mbwee, koma katswiri wa zanthaka kusukulu yaukachenjede ya Chancellor College, Dr Jimmy Namangale,…
Read More » -
Nkhani
Maphunziro a chidyerano cha chimbudzi athandiza
Moyo wasintha ndipo kamphepo kayaziyazi kakudutsa tsopano m’midzi 13 yozungulira dera la T/A Njewa ku Lilongwe anthu atasintha khalidwe lochitira…
Read More » -
Nkhani
Lamulo lochotsa mimba ladengula
… Akufuna ogwiriridwa, opatsana pathupi pachibale ndi ana achichepere aziloledwa kuchotsa pathupi Lamulo lokhudza kuvomereza kuti amayi akhoza kumachotsa…
Read More »