Nkhani
-
Ndikulemba anthu 200—a Mutharika
Mtsogoleri wa dziko lino a Peter Mutharika adzudzula anthu omwe akuti amawanena m’masamba a mchezo kuti sadalingalire amayi posankha maudindo…
Read More » -
Amalawi alankhula pa malonjezo
Amalawi ena ati mpofunika ndondomeko zogwirika kuti boma lomwe lalowa kumene la DPP likwaniritse malonjezo ake a m’manifesto. Ena mwa…
Read More » -
Chitonzo chakula
Mmodzi mwa akadaulo a momwe ziwalo za m’thupi zimagwirira ntchito, physiology, wati chiwerengero cha abambo amene amakayezetsa ngati ali obereka…
Read More » -
Apempha achinyamata asunge bata
Pamene dziko lino likukonzekera kuponya mavoti Lachiwiri likudzali, wapampando wa bungwe la Machinga District Youth Network a Mphatso Chikaonda apempha…
Read More » -
Lorani mtendere ulamulire
Kampeni ikutha mawa. Atsogoleri atambasula mfundo zawo za chitukuko zomwe zili m’manifesto. Nawo mabungwe a Oxfam ndi Women Legal Resource…
Read More » -
Mabungwe akufuna malamulo okhudza AI
Mabungwe a Centre for Human Rights and Rehabilitation (CHRR) ndi Malawi Human Rights Commission (MHRC) apempha boma kuti liunikenso malamulo…
Read More » -
Zikhalidwe zikukhomerera amayi
Wapampando wa Engalaweni Women Group a Mervis Mvula akuti zikhalidwe, zikhulupiriro ndi umphawi ndizo zikulepheretsa amayi ambiri kulowa ndale. A…
Read More » -
Dolo ndi ndani mu chipeta ichi?
Pamene kwatsala masiku atatu okha kuti nzika za dziko lino zivote, atsogoleri omwe akuimira pa mipando ya upulezidenti, uphungu wa…
Read More » -
Kandideti walonjeza nsapato, maendedwe otsika mtengo
Malonjezo pa nthawi ya chisankho si achilendo. Koma pali ena oti ukamva, umagwedeza mutu. Yemwe adzaimire chipani cha UTM ku…
Read More » -
Kandideti wa MCP wapambana anthu asanavote
Bungwe la zachisankho la Malawi Electoral Commission (MEC) lati yemwe amaimira chipani cha Malawi Congress Party (MCP) ku dera la…
Read More »