Nkhani
-
Aika makamera m’ndende
Mabungwe omenyera ufulu wa anthu alandira ndi manja awiri ganizo la nthambi ya za ndende loika makamera m’ndende ngati njira…
Read More » -
Bilu ya CDF yatsamwa
Mabungwe omwe si aboma ayamikira a Pulezidenti a Peter Mutharika pokana kusainira bilu yofuna kuti aphungu aziyendetsa thumba la chitukuko…
Read More » -
Sangalalani mosamala
Pomwe zisangalalo zili mkati, akadaulo achenjeza kuti kusangalala kopanda bajeti ndiko kumachititsa mwezi wa January kukhala wowawa kwa anthu ochuluka…
Read More » -
Adandaula za misewu yosakonzedwa
Pomwe anthu akhala akuitsotsombetsa nthambi ya Road Fund Administration ati ponena kuti ikukanika kukonza misewu ya m’dziko muno chonsecho nthambiyo…
Read More » -
Kungoimvera fungo Khrisimasi
Kwangotsala masiku anayi kuti tsiku limene Akhristu amakumbukira kubadwa kwa Yesu Khristu. Kafungo ka mpunga, nyama yootcha, nkhuku yowiritsa ngakhale…
Read More » -
Gule wamkulu akusokoneza
Atsogoleri omwe anali ku msonkhano wa Unesco wokhudza kuteteza masewera a chikhalidwe adaonetsa kuda nkhawa ndi kukula kwa chiwerengero cha…
Read More » -
Mafumu, a m’boma apezeka mu Fisp
Nduna ya za malimidwe, mthirira ndi chitukuko cha madzi Mayi Roza Mbirizi ati athana ndi ogwira ntchito m’boma omwe ayerekeze…
Read More » -
Bilu ya CDF yadutsa popanda wotsutsa
Aphungu a Nyumba ya Malamulo dzana adutsitsa bilu yomwe akufuna kuti apitirize kuyang’anira zitukuko za ndalama za Constituency Development Fund…
Read More » -
Mabwana a apolisi akana kusamuTsidwa
Bwalo lalikulu la milandu ku Lilongwe laletsa boma kusamutsa akuluakulu a apolisi asanu omwe analamulidwa kuti achoke ku polisiko ndi…
Read More » -
Fisp yabwerera m’bwalo
Mtsogoleri wa dziko lino a Peter Mutharika Lachisanu adalengeza kuti ndondomeko ya zipangizo za ulimi zotsika mtengo yabwerera ku Farm…
Read More »