Nkhani

  • Samalani, kunjaku kwabuka cholera

    Boma lalandira matamando pa momwe layendetsera dziko m’masiku 100 oyambirira koma malesawa akumana n’chipsinjo cha matenda a cholera omwe abuka…

    Read More »
  • Zaka zisanu chifukwa choba katundu

    Bwalo la First Grade Magistrate ku Lilongwe, Lachinayi lidagamula Mayi Esther James a zaka 38 kuti akakhale ku ndende kwa…

    Read More »
  • Aika makamera m’ndende

    Mabungwe omenyera ufulu wa anthu alandira ndi manja awiri ganizo la nthambi ya za ndende loika makamera m’ndende ngati njira…

    Read More »
  • Bilu ya CDF yatsamwa

    Mabungwe omwe si aboma ayamikira a Pulezidenti a Peter Mutharika pokana kusainira bilu yofuna kuti aphungu aziyendetsa thumba la chitukuko…

    Read More »
  • Sangalalani mosamala

    Pomwe zisangalalo zili mkati, akadaulo achenjeza kuti kusangalala kopanda bajeti ndiko kumachititsa mwezi wa January kukhala wowawa kwa anthu ochuluka…

    Read More »
  • Adandaula za misewu yosakonzedwa

    Pomwe anthu akhala akuitsotsombetsa nthambi ya Road Fund Administration ati ponena kuti ikukanika kukonza misewu ya m’dziko muno chonsecho nthambiyo…

    Read More »
  • Kungoimvera fungo Khrisimasi

    Kwangotsala masiku anayi kuti tsiku limene Akhristu amakumbukira kubadwa kwa Yesu Khristu. Kafungo ka mpunga, nyama yootcha, nkhuku yowiritsa ngakhale…

    Read More »
  • Gule wamkulu akusokoneza

    Atsogoleri omwe anali ku msonkhano wa Unesco wokhudza kuteteza masewera a chikhalidwe adaonetsa kuda nkhawa ndi kukula kwa chiwerengero cha…

    Read More »
  • Mafumu, a m’boma apezeka mu Fisp

    Nduna ya za malimidwe, mthirira ndi chitukuko cha madzi Mayi Roza Mbirizi ati athana ndi ogwira ntchito m’boma omwe ayerekeze…

    Read More »
  • Bilu ya CDF yadutsa popanda wotsutsa

    Aphungu a Nyumba ya Malamulo dzana adutsitsa bilu yomwe akufuna kuti apitirize kuyang’anira zitukuko za ndalama za Constituency Development Fund…

    Read More »
Back to top button