Chichewa
-
Akufuna msewu, Admarc ku Tsangano However, the judge found that Chisale’s case did not meet the threshold for certification.
Mfumu yaikulu Mpando ku Ntcheu yalangiza boma kuti liganizire zomanga msika wokhazikika komanso msewu wabwino ku Tsangano m’boma la Ntcheu…
Read More » -
Kandideti walonjeza nsapato, maendedwe otsika mtengo
Malonjezo pa nthawi ya chisankho si achilendo. Koma pali ena oti ukamva, umagwedeza mutu. Yemwe adzaimire chipani cha UTM ku…
Read More » -
Kandideti wa MCP wapambana anthu asanavote
Bungwe la zachisankho la Malawi Electoral Commission (MEC) lati yemwe amaimira chipani cha Malawi Congress Party (MCP) ku dera la…
Read More » -
Aphungu asintha lamulo
Fumbi lakhazikika lokhudza komwe anthu omwe adzakhale akugwira ntchito za chisankho pa nthawi yovota pa September 16 adzaponyere voti yawo.…
Read More » -
MEC yasefa ma kandideti, 17 adutsa
Pomwe kampeni ili mkati, bungwe la Malawi Electoral Commission (MEC) latulutsa maina a ma kandideti omwe akwaniritsa zofunika pa mpando…
Read More » -
Asafuna kusaina pangano osamuvotera
Kampeni ya zisankho za mtsogoleri wa dziko lino, aphungu a Nyumba ya Malamulo ndi makhansala yafika pa mwana wakana phala.…
Read More » -
CDF idatsamwitsa aphungu, makhansala
Pomwe aphungu ndi makhansala amene agwira ntchito yawo kwa zaka 6 akwangula ntchito yawo Lachitatu, akadaulo ndi nzika zina anenetsa…
Read More » -
Miyezi 30 kwa ogona ndi ng’ombe
Bwalo la Chitipa Senior Resident Magistrate, Lolemba pa 14 July 2025, lidagamula bambo wina wa zaka 24 a James Mtambo,…
Read More » -
Adandaula za nyumba ya chisoni
Anthu okhala m’dera la Lisungwi m’boma la Neno adandaula ndi kusagwira ntchito kwa nyumba ya chisoni. Nyumba ya chisoni ya…
Read More » -
Amanga womuganizira kuba chimanga
Bwalo la First Grade Magistrate ku Thyolo masiku apitawa lidagamula bambo Mphatso Mateyu, omwe amachokera m’mudzi mwa Changata, m’dera la…
Read More »