Chichewa
-
Njala saweta, atero kadaulo
Kadaulo pa za malimidwe ndi kuonetsetsa kuti anthu ali nchakudya chokwanira a Tamani Nkhono-Mvula aunikira boma kuti lisamalote pa mpando…
Read More » -
Mpikisano pa usipikala, asankha nduna zina
Pomwe aphungu a Nyumba ya Malamulo ayambe kukumana posakhalitsapa, mpikisano ulipo pofuna kusankha masipikala ngakhalenso aphungu amene akhale m’makomiti. Izi…
Read More » -
Kuteteza chilengedwe
Pomwe vuto la mapulasitiki opyapyala likupitirira kuononga chilengedwe, ophunzira awiri a pa sukulu ya ukachenjede ya Mubas adza ndi mapulasitiki…
Read More » -
Zaka 6 chifukwa choononga njanji
Bwalo la milandu la Second Grade Magistrate m’boma la Dowa lagamula a Laurent Chigowa, a zaka 45 kuti akakhale ku…
Read More » -
Ndikulemba anthu 200—a Mutharika
Mtsogoleri wa dziko lino a Peter Mutharika adzudzula anthu omwe akuti amawanena m’masamba a mchezo kuti sadalingalire amayi posankha maudindo…
Read More » -
Amalawi alankhula pa malonjezo
Amalawi ena ati mpofunika ndondomeko zogwirika kuti boma lomwe lalowa kumene la DPP likwaniritse malonjezo ake a m’manifesto. Ena mwa…
Read More » -
Chitonzo chakula
Mmodzi mwa akadaulo a momwe ziwalo za m’thupi zimagwirira ntchito, physiology, wati chiwerengero cha abambo amene amakayezetsa ngati ali obereka…
Read More » -
TIDAKUMANA: ‘Mudali mu Barbershop’
Lidali tsiku Lachisanu masana m’chaka cha 2012 ku Area 25 C ku Lilongwe ndipo kunja kudali kwa dzuwa pomwe Shingrai…
Read More » -
Apempha achinyamata asunge bata
Pamene dziko lino likukonzekera kuponya mavoti Lachiwiri likudzali, wapampando wa bungwe la Machinga District Youth Network a Mphatso Chikaonda apempha…
Read More » -
Lorani mtendere ulamulire
Kampeni ikutha mawa. Atsogoleri atambasula mfundo zawo za chitukuko zomwe zili m’manifesto. Nawo mabungwe a Oxfam ndi Women Legal Resource…
Read More »