Chichewa
-
Za anamapopa sizikuzilala
Nkhani ya anamapopa ikulephera kutha. Mtsogoleri wa dziko lino Peter Mutharika atangomaliza kuyendera maboma amene anthu angapo aphedwa powaganizira kuti…
Read More » -
Amangidwa popha ‘anamapopa’
Ndende ya Nsanje ikusunga anthu awiri omwe akuyenera kuyankha mlandu wopha Landani Chipira wa zaka 48 atamuganizira kuti ndi ‘namapopa’…
Read More » -
Chipalamba ku Malawi
Dziko la Malawi likusanduka chipalamba. Kafukufuku wathu wapeza kuti mafumu ndi apolisi ena ndiwo akuthandizira kusambula dzikoli pamene akuthandizira kudula…
Read More » -
Bambo amwalira pofuna kulemera
Bambo wina m’boma la Dedza wamwalira atamwa mankhwala oti alemere. “Ukakamwa mankhwalawa, ukafa sabata imodzi. Ukatuluka mphutsi, ndipo akazi awo…
Read More » -
Gule alipo pa 17 October
Zipani za UDF ndi PP zaimika manja kuti sizidzapikisana nawo pamipando ya phungu pachisankho cha chibwereza chimene chikhalepo pa 17…
Read More » -
Pulogalamu ya ECRP yatha
Pulogalamu yophunzitsa anthu kuteteza chilengedwe ya Enhancing Community Resilience Programme (ECRP) yatha itakhalapo zaka 6 ikuphunzitsa anthu m’maboma 7. Mkulu…
Read More » -
Maofesala a kalembera ayera mmanja
Maofesala omwe akugwira ntchito yolembera nzika za dziko lino m’nkalembera wa anthu mwaunyinji ayamba kulandira malipiro awo atsopano. Chiyambireni ntchitoyi…
Read More » -
DPP ikhumudwitsa ku KK
Mafumu ena ku Nkhotakota ndi okwiya ndi chipani cha DPP chimene akuchidzudzula pogwiritsa ntchito galimoto ya chipatala pa ntchito zachipani.…
Read More » -
Njengunje pothana ndi matenda a khansa
Muli ntchito yaikulu m’dziko muno kuti odwala matenda a khansa apeze mpumulo. Izi wanena ndi yemwe adapulumuka ku matendawa, Blandina…
Read More » -
‘Tipulumutseni ku ukwati wa ana’
Amati ana ndi tsogolo la mawa. Koma zikuchitika ku Neno zikukaikitsa ngati adzakhaledi atsogoleri mawa. Kumeneko ukwati wa ana akuti…
Read More »