Chichewa
-
Mphekesera zizunza anthu ku Mangochi
Zina ukamva, kamba anga mwala ndithu. Anthu a m’boma la Mangochi sabata yapitayi adadzuka pakati pausiku, ena m’bandakucha, n’kuyamba kukupa…
Read More » -
A Malawi akufuna 2018 wa ngwiro
Pomwe chaka cha 2018 changoyamba kumene, mtsogoleri wa zipani zotsutsa boma Lazarus Chakwera ndi akadaulo ena ati boma lisinthe kayendetsedwe…
Read More » -
‘ankawerenga nkhani pa mij’
Ndi mawu okha, MarcFarlane Mbewe wa Capital Radio adachiritsidwa. Awa ndi makumanidwe a mnyamatayu ndi Lisa Lamya, mtolankhani wa Yoneco…
Read More » -
Ndewu ya gule kudambwe
Kudali fumbi koboo! Kudambwe la Phingo m’boma la Chikwawa pamene gulewamkulu adaponyerana zibakera pokanganirana zovala zovinira. Mneneri wapolisi ya Chikwawa…
Read More » -
‘Osalanga nokha oganiziridwa ufiti’—Apolisi
Anthu m’mudzi mwa Chimchembere kwa T/A Chekucheku m’boma la Neno adavomera mwa mphamvu kuti ufiti ulipo, makamaka mphenzi zopanga anthu.…
Read More » -
Kuli zionetsero pa 13 December
Lachitatu pa 13 December kukhala ali ndi mwana agwiritse m’zigawo zonse zitatu za dziko lino pamene bungwe la mipingo la…
Read More » -
‘Mafumu adyera’
Akatswiri pandale komanso mafumu adzudzula zomwe adachita mafumu ena poyenda ndawala ulendo ku Nyumba ya Malamulo komwe amakatsutsa mabilo a…
Read More » -
Rasta akaseweza zaka 6
Mlandu woba njinga komanso kulasa ndi mpeni paphuzi pa bambo wa kabaza, watumiza Fedson Missi kundende komwe akaseweze zaka 6.…
Read More » -
Malawi ali mu mdima
Zasokonekera! Malawi ali pamoto wosaneneka ndi kuzimazima kwa magetsi. Anthu akumudzi akugona kuchigayo kudikira magetsi pamene alimi a ng’ombe zamkaka…
Read More » -
‘Timakaonera masewero a mpira’
Masewero a pakati pa Police Secondary School ndi St Paul Private Secondary ku Zomba adzakhala chikumbutso kwa Owen Chaima, kuti…
Read More » -
Malawi ali mumdima wa dzaoneni
Dziko la Malawi laona mdima womwe sudaonekepo chilandirireni ufulu wodziyimira palokha. Madera ena akukhala masiku awiri magetsi osayaka. Kwina, ndiye…
Read More » -
Pac iwopseza boma pa bilo yachisankho
Lisafike Lachitatu sabata ya mawa musanabweretse bilo yokhudza chisankho ndi maboma ang’ono. Latero bungwe la amipingo la Public Affairs Committee…
Read More » -
Matafale memorial shows under threat
It is Wednesday. Four days before the annual Evison Matafale Memorial Show in Blantyre. But the Black Missionaries are yet…
Read More » -
Zipani zikufuna mayankho pa zitupa za unzika
Zipani za Malawi Congress Party (MCP) ndi People’s Party (PP) zati kusowa kwa zitupa zina za olembetsa m’kaundula wa unzika…
Read More » -
Zitupa zaunzika zina zasowa
Zitupa 93 893 za uzika m’boma la Kasungu zasowa. Tamvani itha kuvumbulutsa. Izitu zadziwika pamene bungwe lolembera unzika la National…
Read More » -
Achita zionetsero za kuthimathima kwa magetsi
Anthu okhudzidwa a mu mzinda wa Lilongwe adachita ziwonetsero zosonyeza kukwiya kwawo ndi kuthimathima kwa magetsi m’dziko muno. Cholinga cha…
Read More » -
‘Boma likutengera a Malawi kumtoso’
Pamene nkhani ya malamulo oyendetsera zisankho ili mkamwamkamwa, mkulu womenyera ufulu wa anthu, John Kapito, wati nkhani za magetsi, madzi…
Read More » -
Titsirika nkhalango zonse—Ng’anga
Gulu lina la asing’anga ku Dedza ladzithemba kuti likhoza kuteteza nkhalango za dziko lino ndi chambu koma akuluakulu a boma…
Read More » -
Makuponi n’chipsinjo—Mafumu
Kuchepa kwa makuponi ogulira zipangizo za ulimi zotsika mtengo omwe boma limagawa kwa anthu mogwirizana ndi mafumu, kukubweretsa chitonzo kwa…
Read More » -
Tambala wameza chimanga
Kusadabuzika kwa chipani cha DPP pa chisankho chapadera kukutanthauza kuti Amalawi atopa ndi ulamuliro wa chipanicho, akadaulo a ndale ena…
Read More »