Nkhani
-
Mukufuna kulima chamba?
Kwa nthawi yaitali, chamba chakhala chikulimidwa m’dziko muno mozembera malamulo. Komatu makono kwadza chamba chosazunguza bongo chimene akuchitama kuti chikhonza…
Read More » -
Anthu ochuluka akufuna katemera
Pomwe zipatala zambiri zayamba kubaya katemera woteteza ku matenda a Corona mu gawo loyamba, achipatala ati anthu ankhaninkhani omwe sali…
Read More » -
Zokolola zichuluka
Unduna wa zamalimidwe wati chaka chino dziko la Malawi likolola chimanga chokwana matani 4.4 miliyoni chomwe nchopitilira mlingo omwe dziko…
Read More » -
Tikwanitsa lonjezo lililonse—Chakwera
Mtsogoleri wadziko lino Lazarus Chakwera wati Amalawi asamvere za anthu omwe akufalitsa kuti boma lake lafotsera malonjezo omwe lidapereka pa…
Read More » -
Kutakata ndi ulimi wa mitengo ya zipatso
Pamene alimi ena akukangalika ndi ulimi wa ziweto kapena mbewu zina, Pilirani Tendai Khoza adapeza mtaji pa ulimi wa mitengo…
Read More » -
Zigamulo zogwirira zikufooketsa
Sabata yatha inali imodzi mwa sabata yomwe inaika pa mbalambanda kuya kwa nkhani zogwiririra m’dziko muno. Pomwe bambo wina wa…
Read More » -
Akana ndalama za Covid-19
Anthu ayera m’manja. Ndalama za Covid zatuluka. Komatu mayi wina mumzinda wa Mzuzu wakana kulandira ndalamazi akuti nzasataniki. Mayiyo akuti…
Read More » -
Mipingo yakonzeka zophunzitsa anthu za katemera wa Covid 19
Thunthu loyamba la katemera wa Covid 19 lidafika mziko muno sabata ikuthayi ndipo malingana ndi mtsogoleri wa dziko lino Lazarus…
Read More » -
Boma ligulitsa chimanga pamtengo wa sabuside
Kadaulo pazamalimidwe Tamani Nkhono-Mvula wati boma likhale ndi ndondomeko yokhwima yogulitsira chimanga pa mtengo wa sabuside ngati momwe lakonzera poopa…
Read More » -
Mtsutso pa zoika a Covid-19
Kusamvana kukupitirira pakati pa achipatala ndi anthu pa ndondomekoyoyenera kutsatidwa munthu yemwe amadwala matenda a Covid-19 akamwalira. Pomwe achipatala akuti…
Read More »