Nkhani
-
‘Osakondera odya nawo K6.2 biliyoni’
Bota layamba kuwira mumphika wa K6.2 biliyoni yothandiza polimbana ndi matenda a Covid 19 yomwe ikumveka kuti idatafunidwa ndipo akuluakulu…
Read More » -
Sukulu zitsegulidwanso
Mkokemkoke umene udalipo pakati pa aphunzitsi ndi boma watha tsopano ndipo ophunzira amayenera kubwerera kusukulu dzulo Lachisanu. Izi zadza kutsatira…
Read More » -
Ayamikira boma pa ganizo lotsegulanso sukulu
Komiti yotsogolera kulimbana ndi matenda a Covid yalengeza kuti sukulu zonse zitsegulidwe Lolemba likudzali pa 22 February. Nduna ya zaumoyo…
Read More » -
Aphungu akumana lolemba
Aphungu a Nyumba ya Malamulo ayamba kuunika momwe bajeti ya 2020 mpaka chaka chino yayendera m’miyezi 6 yoyamba Lolemba likudzali…
Read More » -
Mtsutso pa zotsegulira sukulu lolemba
Pulani ya boma yoti sukulu zikuyenera kutsegulidwanso Lolemba likudzali yasinthidwanso ndipo tsopano Unduna wa zamaphunziro ukufuna kuti uwunikenso m’mene mliri…
Read More » -
Akhumudwa ndi kusowa kwa mnyamata wachialubino
Magulu omenyera ufulu wa anthu komanso bungwe la anthu achialubino la Association for People with Albinism in Malawi (Apam) ati…
Read More » -
Zisangalalo zafika, samalani
Yafika nyengo ya zisangalalo za Khrisimasi ndi Nyuwere ndipo ena ayamba kale mapwando pomwe ena akukonzekera masangalalidwe osiyanasiyana monga kupita…
Read More » -
Mademo ayambika
Gulu lomwe lakhala likudzudzula boma la Tonse Alliance chilowereni m’bomamo la Centre for Democracy and Economic Development Initiative (Cdedi) mogwirizana…
Read More » -
Makhansala aderera alawansi
Kucha kwa Lolemba lapitali Amalawi adadzuka ndi nkhani yododometsa kuona adindo (makhansala) akulalata poyera kudelera alawansi ya K20 000 ndipo…
Read More » -
Athotha a kabaza opanda mapepala
Boma lalamula apolisi m’dziko muno kuti athothe akabaza onse a njinga zamoto zopanda mapepala oziyenereza kuyenda pamsewu ndi kumanyamula anthu.…
Read More »