Nkhani
-
Mgwirizano wabooka?
Amati “apolisi tisamawanyoze ndi abale athu”, koma zayambika m’dziko muno ndi chipolowe pamene anthu akuthotha apolisi ndi kusasula ofesi zawo…
Read More » -
Womukaikira zopakula ku Kapitolo adzipereka
Wabizinesi Osward Lutepo, amene wakhala akusakidwa ndi apolisi a dziko lino, komanso polisi ya maiko osiyanasiyana ya Interpol, Lachitatu adatera…
Read More » -
Kupha nyani sayang’ana nkhope
Kuyambira pomwe dziko lino lidayamba kukhala ndi ulamuliro wa demokalase (matipate) zinthu pang’onopang’no zidayamba kusokonekera, makamaka pakayendetsedwe ka chuma. Muulamuliro…
Read More » -
Umphawi ulikonso kutauni—mtsutso
Ngati munali ndi malingaliro oti muchoke kumudzi ndi kukatambalala kutauni kuti mwina ndiko kuli msipu wobiriwira, iwalani ndithu chifukwa kumeneko…
Read More » -
Kodi za Gaba zalowa?
M’sabatayi aganyu tidali osangalala kumva kuti chilombo cha ukonde, Gabadihno Mhango, mwana wa Flames, tsopano wayamba kusewerera m’timu yatsopano ya…
Read More » -
Kusolola m’boma kudayamba kale
Zayamba kuululika. Kafukukufuku yemwe adapangidwa pakati pa 2009 ndi 2012 waulula kuti boma lotsogozedwa ndi chipani cha DPP, chomwe mtsogoleri…
Read More » -
Kampani yatsopano ikatamutsa alimi
Kampani yatsopano yogula ndi kugulitsa zakumunda ya Auction Holdings Limited Commodities Exchange (AHCX) yamema alimi kuti akagulitse mbewu zawo kubungweli…
Read More » -
Kugwiririra ana kudzatha?
Pafupufupi tsiku lililonse tikumamva kapena kuwerenga malipoti akuti mwana wagwiririridwa penapake. Omangidwa akumangidwa. Kugwira ndende ndiye kosakamba koma zikuoneka kuti…
Read More » -
Kupakula kukapitolo, JB achotsa nduna
Mtsogoleri wadziko lino Joyce Banda Lachitatu adakana kupumitsa mamulumuzana ena aboma kutsatira kupakula ndalama za boma kumene kwanyanya kulikulu la…
Read More » -
A ku Mozambique akulembetsa mavoti
Nzika zina za m’dziko la Mozambique zikulembetsa nawo m’kaundula wa mavoti ku Dedza popofuna kuti zidzavote nawo pa chisankho cha…
Read More »