Nkhani
-
Ine ayi, Dausi wakana Chaponda
Zomwe zachitika ku bwalo la mirandu ku Lilongwe m’sabatayi zalephera kupherezera mwambi woti khoswe akakhala pa mkhate sapheka. Khwimbi…
Read More » -
Ulendo wa chisankho wapsa
Zipani zina zati bungwe loyendetsa chisankho la Malawi Electoral Commission (MEC) liyenera kukwaniritsa zomwe lidalonjeza sabata yatha kuti chisankho cha…
Read More » -
Zikhulupiriro zikufalitsa kolera—unduna
Unduna wa zaumoyo wati zikhulupiriro ndizo zikuchititsa kuti chiwerengero odwala kolera chizikwera. Koma bungwe la United Nations Children’s Fund (Unicef)…
Read More » -
Chitetezo chaphwasuka
Chitetezo chaphwasuka. Anthu akuberedwa, kumenyedwa ndi kuchitidwa zachipongwe zambiri. Akaitanitsa apolisi akuti akumatenga nthawi kuti abwera ndipo nthawi zina sabwera.…
Read More » -
Kolera yaluma mano
Nthenda ya kolera imene idayamba ngati njerengo mwezi wa November chaka chatha, ikukwererabe moti kuchoka Lachisanu sabata yatha chiwerengero…
Read More » -
Kalembera wa mafoni aima
Boma laimitsa kalembera wa lamya za m’manja yemwe nthambi yoyendetsa ntchito za mauthenga ya Malawi Communications Regulatory Authority (Macra) idakhazikitsa…
Read More » -
Chilimikani pa ulimi—Kazembe
Malinga ndi ng’amba imene yasautsa m’madera ambiri m’dziko lino, wachiwiri kwa kazembe wa limodzi mwa maiko a ku Ulaya la…
Read More » -
MEC ikufunakusinthatsiku la chisankho
Pavuta kuti chisankho chichoke mwezi wa May kupita September monga bungwe loyendetsa chisankho la Malawi Electoral Commission (MEC) lidapemphera komitiya…
Read More » -
Osinthasintha zipani ngosadalilika—Akadaulo
Andale osinthasintha zipani ndi osadalilika, ndipo amachita izi chifukwa cha dyera, atero akadaulo ena a zandale. Koma ena mwa andalewo…
Read More » -
Kwadza kaundula wa foni za m’manja
Eni lamya za m’manja m’dziko muno akuyenera kulowa m’kaundula wa umwini wa lamya zawo kuti azitha kugwiritsa ntchito lamya zawozo,…
Read More »