Nkhani
-
Akufuna boma lichitepo kanthu pa za zigandanga
Akadaulo oimira magulu osiyanasiyana ati boma likuyenera kuchitapo kanthu pa za zigandanga za zikwanje zomwe zakhala zikusokoneza zionetsero osati kungolankhulapo…
Read More » -
‘Si ife oyendayenda’
Amayi amene ali ndi mwana kapena ana koma si ali pa banja si mahule, momwe ena amaganizira, watero mlembi komanso…
Read More » -
Apempha kafukufuku pa CDF
Pomwe chiwerengero cha anthu maka abambo odzipha chikupitirira kukwera m’dziko nacho chiwerengero cha achinyamata makamaka omwe ali sukulu za ukachenjede…
Read More » -
6 July ili ku BNS
Nduna ya zofalitsa nkhani a Moses Kunkuyu apempha Amalawi amene akudzapita ku chisangalalo choti dziko lino lakwanitsa zaka 61 lili…
Read More » -
Namiwa alira: dzikoli lafika apa?
Patangotha masiku atatu akuluakulu a nthambi za chitetezo atasankha atsogoleri a za chitetezo pomwe dziko lino likukonzekera Chisankho Chachikulu pa…
Read More » -
Imfa ya wa kabanza
Anthu okwiya m’taunishipi ya Machinjiri mu mzinda wa Blantyre aphwanya mazenera ndi zitseko za polisi yaing’ono ya Nanthoka ndi kuotcha…
Read More » -
Wakuba ufa ndi makala agamulidwa zaka 4
Bambo Cosmas Chiwambo, a zaka 22, omwe amachokera m’mudzi mwa Mwamadi kwa T/A Chikumbu m’boma la Mulanje, alamulidwa kuti akakhale…
Read More » -
Amanga oba zitsulo pa mlatho
Apolisi m’boma la Mulanje atsekera m’chitokosi abambo anayi powaganizira kuti adaba zitsulo za pa mlatho wopezeka m’dera la kummwera cha…
Read More » -
Akachasu nawo akulira ndi kukwera kwa shuga
Mwina n’kumaona ngati amene amakonda za tseketseke monga tiyi ndi makeke okha ndi amene akulira ndi kusowa komanso kukwera mtengo…
Read More » -
Kusamvana pa mwambo wokumbukira Chilima
Mwambo wokumbukira yemwe adali mtsogoleri wakale wa dziko lino a Saulos Chilima uchitika Lachiwiri likudzali kwawo ku Nsipe komwe thupi…
Read More »